Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 33:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiyeno anawonjezera kuti: “Sungathe kuona nkhope yanga, chifukwa palibe munthu amene angandione nʼkukhalabe ndi moyo.”

  • Yohane 1:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Palibe munthu amene anaonapo Mulungu ndi kale lonse,+ mulungu wobadwa yekha+ amene ali pambali pa Atate*+ ndi amene anafotokoza za Mulungu.+

  • Yohane 4:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mulungu ndi Mzimu,+ ndipo amene akumulambira akuyenera kumulambira motsogoleredwa ndi mzimu komanso choonadi.”+

  • Yohane 6:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Palibe munthu amene anaonapo Atate,+ kupatulapo yekhayo amene anachokera kwa Mulungu, ameneyu anaona Atate.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena