Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aefeso 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Valani zida zonse zankhondo+ zochokera kwa Mulungu kuti musagonje polimbana ndi zochita zachinyengo* za Mdyerekezi,

  • 1 Timoteyo 1:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mwana wanga Timoteyo, ndikukulangiza kuchita zimenezi mogwirizana ndi maulosi amene ananeneratu za iwe, kuti mogwirizana ndi maulosiwo upitirize kumenya nkhondo yabwino.+ 19 Ukhale ndi chikhulupiriro komanso chikumbumtima chabwino+ chimene anthu ena asiya kuchitsatira, moti chikhulupiriro chawo chasweka ngati ngalawa.

  • 1 Timoteyo 6:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Menya nkhondo yabwino ya chikhulupiriro. Gwira mwamphamvu moyo wosatha umene anakuitanira. Paja unalengeza momveka bwino zokhudza moyo umenewu pamaso pa mboni zambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena