Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ine Yehova ndalankhula. Zimene ndidzachitire gulu lonse la anthu oipali, amene asonkhana kuti atsutsane ndi ine ndi izi: Onse adzafera mʼchipululu muno ndipo adzathera momwe muno.+

  • 1 Akorinto 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano abale, ndikufuna mudziwe kuti makolo athu akale, onse anali pansi pa mtambo+ ndipo onse anawoloka nyanja.+

  • 1 Akorinto 10:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ngakhale zinali choncho, ambiri a iwo Mulungu sanakondwere nawo ndipo anaphedwa mʼchipululu.+

  • Aheberi 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kodi paja ndi ndani amene anamva koma nʼkupsetsa mtima Mulungu? Kodi si anthu onse amene anatuluka mʼdziko la Iguputo motsogoleredwa ndi Mose?+

  • Aheberi 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Choncho, tikuona kuti sakanatha kulowa mumpumulowo chifukwa anali opanda chikhulupiriro.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena