Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 8:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma zogwera panthaka yabwino, ndi anthu amene pambuyo pomva mawuwo ndi mtima wabwino kwambiri,+ amawagwiritsitsa nʼkubereka zipatso mopirira.+

  • Luka 21:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ngati inu mudzapirire, mudzapeza moyo.+

  • 2 Timoteyo 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tikapitiriza kupirira, tidzalamuliranso naye monga mafumu.+ Tikamukana, iyenso adzatikana,+

  • Aheberi 10:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Mukufunika kukhala opirira+ komanso kuchita chifuniro cha Mulungu kuti mudzalandire zimene Mulunguyo walonjeza.

  • Aheberi 12:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho ganizirani mozama za munthu amene anapirira malankhulidwe onyoza amenewo a anthu ochimwa,+ amene polankhula zimenezo ankangodzivulaza okha. Ganizirani za munthu ameneyu kuti musatope nʼkutaya mtima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena