Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 2:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kukhala Myuda weniweni kuli mumtima+ ndipo mdulidwe wake umakhalanso wamumtima+ wochitidwa ndi mzimu, osati ndi malamulo olembedwa.+ Munthu woteroyo amatamandidwa ndi Mulungu, osati anthu.+

  • Aroma 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Komabe sizikutanthauza kuti mawu a Mulungu sanakwaniritsidwe. Chifukwa si onse omwe ndi mbadwa za Aisiraeli amene alidi “Aisiraeli.”+

  • Agalatiya 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma onse amene amatsatira lamulo limeneli la mmene tiyenera kukhalira, amene ndi Isiraeli wa Mulungu,+ akhale ndi mtendere ndipo Mulungu awasonyeze chifundo.

  • Chivumbulutso 21:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mzindawo unali ndi mpanda waukulu komanso wautali ndipo unali ndi mageti 12. Pamagetiwo panali angelo 12 ndipo panalembedwa mayina a mafuko 12 a ana a Isiraeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena