Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 75:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Mʼdzanja la Yehova muli kapu.+

      Vinyo akuchita thovu ndipo wasakanizidwa bwino.

      Ndithudi, iye adzakhuthula vinyo yense

      Ndipo anthu onse oipa padziko lapansi adzamwa mpaka kugugudiza nsenga zake.”+

  • Chivumbulutso 11:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Koma mitundu ya anthu inakwiya ndipo inunso munasonyeza mkwiyo wanu. Ndiye nthawi yoikidwiratu inafika yoti akufa aweruzidwe nʼkupereka mphoto+ kwa akapolo anu aneneri+ komanso kwa oyera ndi amene akuopa dzina lanu, olemekezeka ndi onyozeka omwe. Komanso nthawi yoti muwononge amene akuwononga dziko lapansi.”+

  • Chivumbulutso 16:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mzinda waukulu+ unagawika zigawo zitatu ndipo mizinda ya mitundu ya anthu inagwa. Ndiyeno Mulungu anakumbukira Babulo Wamkulu,+ kuti amupatse kapu imene inali ndi vinyo wa mkwiyo wake waukulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena