Deuteronomo 32:43 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 43 Inu anthu a mitundu ina, sangalalani limodzi ndi anthu ake,+Chifukwa adzabwezera magazi a atumiki ake,+Ndipo adzabwezera chilango kwa adani ake,+Komanso adzaphimba machimo a dziko la anthu ake.”* 2 Mafumu 9:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Ukaphe anthu a mʼbanja la mbuye wako Ahabu ndipo ine ndidzabwezera magazi a atumiki anga aneneri ndiponso magazi a atumiki onse a Yehova amene Yezebeli anawapha.+ Salimo 79:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Musalole kuti anthu a mitundu ina azinena kuti: “Mulungu wawo ali kuti?”+ Anthu a mitundu ina adziwe ife tikuonaKuti mwabwezera magazi a atumiki anu amene anakhetsedwa.+ Chivumbulutso 18:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Sangalalani kumwambako chifukwa cha zimene zamuchitikira.+ Inunso oyera,+ atumwi ndi aneneri, sangalalani chifukwa Mulungu wamupatsa chilango chifukwa cha zomwe anakuchitirani.”+ Chivumbulutso 18:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Mwa iye munapezeka magazi a aneneri, a oyera,+ ndi a onse amene anaphedwa padziko lapansi.”+
43 Inu anthu a mitundu ina, sangalalani limodzi ndi anthu ake,+Chifukwa adzabwezera magazi a atumiki ake,+Ndipo adzabwezera chilango kwa adani ake,+Komanso adzaphimba machimo a dziko la anthu ake.”*
7 Ukaphe anthu a mʼbanja la mbuye wako Ahabu ndipo ine ndidzabwezera magazi a atumiki anga aneneri ndiponso magazi a atumiki onse a Yehova amene Yezebeli anawapha.+
10 Musalole kuti anthu a mitundu ina azinena kuti: “Mulungu wawo ali kuti?”+ Anthu a mitundu ina adziwe ife tikuonaKuti mwabwezera magazi a atumiki anu amene anakhetsedwa.+
20 Sangalalani kumwambako chifukwa cha zimene zamuchitikira.+ Inunso oyera,+ atumwi ndi aneneri, sangalalani chifukwa Mulungu wamupatsa chilango chifukwa cha zomwe anakuchitirani.”+