Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chivumbulutso 1:13-15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pakati pa zoikapo nyalezo, panali wina wooneka ngati mwana wa munthu+ atavala chovala chofika kumapazi ndipo anali atamanga lamba wagolide pachifuwa. 14 Komanso, mutu ndi tsitsi lake zinali zoyera ngati ubweya woyera wa nkhosa, zinali zoyera kwambiri, ndipo maso ake anali ngati lawi la moto.+ 15 Mapazi ake anali ngati kopa* woyengedwa bwino+ amene akunyezimira mʼngʼanjo ndipo mawu ake ankamveka ngati mkokomo wa madzi ambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena