Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 16
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Zimene Zili Mʼbuku la Deuteronomo

      • Pasika; Chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa (1-8)

      • Chikondwerero cha Masabata (9-12)

      • Chikondwerero cha Misasa (13-17)

      • Kusankha oweruza (18-20)

      • Zinthu zosayenera kuzilambira (21, 22)

Deuteronomo 16:1

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Zakumapeto B15.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 12:14; Le 23:5; Nu 9:2; 28:16; 1Ak 5:7
  • +Eks 34:18

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Baibulo la Dziko Latsopano (nwt), ptsa. 2136, 2244

Deuteronomo 16:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 26:17
  • +Eks 12:5, 6; 2Mb 35:7
  • +1Mf 8:29

Deuteronomo 16:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 13:3; Le 23:6; Nu 28:17; 1Ak 5:8
  • +Eks 12:33
  • +Eks 12:14; 13:8, 9

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/1990, ptsa. 16-17

Deuteronomo 16:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 12:15; 13:7
  • +Eks 12:10; 34:25

Deuteronomo 16:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 12:3, 6; Nu 9:2, 3; Mt 26:19, 20

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/1990, ptsa. 13-14

Deuteronomo 16:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 12:8; 2Mb 35:13
  • +Yoh 2:13; 11:55

Deuteronomo 16:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 12:16; Le 23:8

Deuteronomo 16:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:16; 34:22; Le 23:15

Deuteronomo 16:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 28:26
  • +De 16:17; 1Ak 16:2; 2Ak 8:12

Deuteronomo 16:11

Mawu a M'munsi

  • *

    Mʼchilankhulo choyambirira, “mʼmageti anu.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 12:5-7

Deuteronomo 16:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 3:7; De 5:15

Deuteronomo 16:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:16; Le 23:34; Nu 29:12; De 31:10, 11; Yoh 7:2

Deuteronomo 16:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 12:12; Ne 8:10, 17; Mla 5:18

Deuteronomo 16:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 23:36, 40; Ne 8:18
  • +De 7:13; 28:8; 30:16
  • +Afi 4:4; 1At 5:16

Deuteronomo 16:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:14, 15
  • +De 16:10
  • +De 16:13

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    3/2022, ptsa. 22-24

    Nsanja ya Olonda,

    3/1/1998, ptsa. 8-9

    9/15/1995, tsa. 22

Deuteronomo 16:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ak 8:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 46

    Ufumu wa Mulungu Ukulamulira, ptsa. 196-197

Deuteronomo 16:18

Mawu a M'munsi

  • *

    Mʼchilankhulo choyambirira, “mʼmageti anu onse amene.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 18:25, 26; De 1:16; 2Mb 19:4, 5

Deuteronomo 16:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:2; Le 19:15
  • +De 1:17
  • +Eks 23:8; 1Sa 12:3; Mla 7:7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/1989, tsa. 12

Deuteronomo 16:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mik 6:8

Deuteronomo 16:21

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Matanthauzo a Mawu Ena.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:13

Deuteronomo 16:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:24; Le 26:1; De 12:3

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 16:1Eks 12:14; Le 23:5; Nu 9:2; 28:16; 1Ak 5:7
Deut. 16:1Eks 34:18
Deut. 16:2Mt 26:17
Deut. 16:2Eks 12:5, 6; 2Mb 35:7
Deut. 16:21Mf 8:29
Deut. 16:3Eks 13:3; Le 23:6; Nu 28:17; 1Ak 5:8
Deut. 16:3Eks 12:33
Deut. 16:3Eks 12:14; 13:8, 9
Deut. 16:4Eks 12:15; 13:7
Deut. 16:4Eks 12:10; 34:25
Deut. 16:6Eks 12:3, 6; Nu 9:2, 3; Mt 26:19, 20
Deut. 16:7Eks 12:8; 2Mb 35:13
Deut. 16:7Yoh 2:13; 11:55
Deut. 16:8Eks 12:16; Le 23:8
Deut. 16:9Eks 23:16; 34:22; Le 23:15
Deut. 16:10Nu 28:26
Deut. 16:10De 16:17; 1Ak 16:2; 2Ak 8:12
Deut. 16:11De 12:5-7
Deut. 16:12Eks 3:7; De 5:15
Deut. 16:13Eks 23:16; Le 23:34; Nu 29:12; De 31:10, 11; Yoh 7:2
Deut. 16:14De 12:12; Ne 8:10, 17; Mla 5:18
Deut. 16:15Le 23:36, 40; Ne 8:18
Deut. 16:15De 7:13; 28:8; 30:16
Deut. 16:15Afi 4:4; 1At 5:16
Deut. 16:16Eks 23:14, 15
Deut. 16:16De 16:10
Deut. 16:16De 16:13
Deut. 16:172Ak 8:12
Deut. 16:18Eks 18:25, 26; De 1:16; 2Mb 19:4, 5
Deut. 16:19Eks 23:2; Le 19:15
Deut. 16:19De 1:17
Deut. 16:19Eks 23:8; 1Sa 12:3; Mla 7:7
Deut. 16:20Mik 6:8
Deut. 16:21Eks 34:13
Deut. 16:22Eks 23:24; Le 26:1; De 12:3
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 16:1-22

Deuteronomo

16 “Muzikumbukira kuti mwezi wa Abibu* ndi wofunika ndipo muzichita chikondwerero cha Pasika kwa Yehova Mulungu wanu,+ chifukwa mʼmwezi wa Abibu Yehova Mulungu wanu anakutulutsani mu Iguputo usiku.+ 2 Ndipo muzipereka nsembe ya Pasika kwa Yehova Mulungu wanu.+ Muzipereka nkhosa ndi ngʼombe+ pamalo amene Yehova adzasankhe kuikapo dzina lake.+ 3 Musamadye nsembeyo limodzi ndi chilichonse chokhala ndi zofufumitsa.+ Kwa masiku 7 muzidya mkate wopanda zofufumitsa, umene ndi mkate wamasautso, chifukwa munatuluka mofulumira mʼdziko la Iguputo.+ Muzichita zimenezi kuti muzikumbukira tsiku limene munatuluka mʼdziko la Iguputo, masiku onse a moyo wanu.+ 4 Musamapezeke ndi mtanda wa ufa wokanda wokhala ndi zofufumitsa mʼdziko lanu lonse kwa masiku 7.+ Nyama iliyonse imene mwapereka nsembe madzulo, pa tsiku loyamba, isamagone mpaka mʼmawa.+ 5 Simudzaloledwa kupereka nsembe ya Pasika mumzinda wanu uliwonse umene Yehova Mulungu wanu akukupatsani. 6 Koma muzidzapereka nsembe ya Pasikayo pamalo amene Yehova Mulungu wanu adzasankhe kuikapo dzina lake. Muzidzapereka nsembeyo madzulo, dzuwa likangolowa,+ pa nthawi yofanana ndi imene munatuluka mu Iguputo. 7 Muzidzaiwotcha nʼkuidya+ pamalo amene Yehova Mulungu wanu adzasankhe,+ ndipo mʼmawa mwake muzidzabwerera kumatenti anu. 8 Muzidya mkate wopanda zofufumitsa kwa masiku 6, ndipo pa tsiku la 7 muzichitira Yehova Mulungu wanu msonkhano wapadera. Pa tsikuli musamagwire ntchito.+

9 Muziwerenga masabata 7. Muziyamba kuwerenga masabata 7 amenewo kuchokera pa nthawi imene mwayamba kumweta tirigu.+ 10 Ndiyeno muzichitira Yehova Mulungu wanu Chikondwerero cha Masabata,+ popereka nsembe zaufulu zimene mungathe, mogwirizana ndi mmene Yehova Mulungu wanu wakudalitsirani.+ 11 Ndipo muzidzasangalala pamaso pa Yehova Mulungu wanu, inuyo, mwana wanu wamwamuna, mwana wanu wamkazi, kapolo wanu wamwamuna, kapolo wanu wamkazi, Mlevi amene akukhala mumzinda wanu,* mlendo amene akukhala pakati panu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye, amene ali pakati panu. Muzidzasangalala pamalo amene Yehova Mulungu wanu adzasankhe kuikapo dzina lake.+ 12 Muzikumbukira kuti munali akapolo ku Iguputo,+ ndipo muzisunga komanso kutsatira malamulo amenewa.

13 Muzichita Chikondwerero cha Misasa+ kwa masiku 7, mukamatuta zokolola kuchokera pamalo opunthira mbewu, pamalo oyengera mafuta ndi pamalo opondera mphesa. 14 Muzisangalala pa chikondwerero chimenecho,+ inuyo, mwana wanu wamwamuna, mwana wanu wamkazi, kapolo wanu wamwamuna, kapolo wanu wamkazi, Mlevi, mlendo amene akukhala pakati panu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye, amene ali mumzinda wanu. 15 Muzichitira Yehova Mulungu wanu chikondwerero chimenecho kwa masiku 7+ pamalo amene Yehova adzasankhe. Muzichita chikondwererochi chifukwa Yehova Mulungu wanu adzadalitsa zokolola zanu zonse ndi chilichonse chimene dzanja lanu likuchita,+ ndipo inu mudzakhala osangalala kwambiri.+

16 Mwamuna aliyense pakati panu azikaonekera katatu pa chaka pamaso pa Yehova Mulungu wanu, pamalo amene Mulungu adzasankhe. Azikaonekera pa Chikondwerero cha Mkate Wopanda Zofufumitsa,+ Chikondwerero cha Masabata+ ndi pa Chikondwerero cha Misasa.+ Palibe aliyense wa iwo amene akuyenera kukaonekera kwa Yehova chimanjamanja. 17 Mphatso imene aliyense ayenera kubweretsa izikhala yogwirizana ndi madalitso amene Yehova Mulungu wanu wakupatsani.+

18 Musankhe oweruza+ ndi atsogoleri a fuko lililonse mʼmizinda yonse imene* Yehova Mulungu wanu akukupatsani ndipo aziweruza anthu mwachilungamo. 19 Musamakhotetse chilungamo,+ musamakondere+ kapena kulandira chiphuphu, chifukwa chiphuphu chimachititsa khungu maso a anthu anzeru+ komanso kupotoza mawu a anthu olungama. 20 Muzichita zinthu mwachilungamo+ kuti mukhale ndi moyo nʼkukatenga dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani.

21 Musadzadzale mtengo uliwonse kuti ukhale mzati wopatulika*+ pafupi ndi guwa lansembe la Yehova Mulungu wanu limene mudzapange.

22 Ndipo musadzaimike chipilala chopatulika,+ chinthu chimene Yehova Mulungu wanu amadana nacho.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena