Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g87 9/8 tsamba 32
  • Mmene Ukwati Umodzi Unapulumutsidwira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mmene Ukwati Umodzi Unapulumutsidwira
  • Galamukani!—1987
Galamukani!—1987
g87 9/8 tsamba 32

Mmene Ukwati Umodzi Unapulumutsidwira

“Kugwiritsira ntchito uphungu wopezedwa mu bukhu la Kupangitsa Moyo Wanu Wabanja Kukhala Wachimwemwe kunapulumutsa ukwati wanga,” analemba motero m’ŵerengi woyamikira kuchokera ku South Africa. “Mutu 5, ‘Mkazi Amene Ali Wokondedwa Kwambiri,’ unatsegula maso anga. Sindinalingalirepo m’maloto anga a akulu kuti ndingapangitse mavuto ambirimbiri popanda kulingalira. Ndikuyamikani kwenikweni. Ukwati wanga unali m’mbali za namondwe zenizeni za nyanja, ndipo tsopano, pambuyo pa miyezi ingapo, iwo wabwereranso kudokho lachimwemwe.”

Ngati mufuna thandizo la kupangitsa ukwati wanu kukhala wachimwemwe, inu mungapindule kuchokera ku bukhu limeneli. Landirani kope limodzi mwakungodzaza ndi kutumiza kapepala kali pansipa.

Chonde tumizani, mutalipiriratu positi, bukhu la chikuto cholimba, la masamba 192 Kupangitsa Moyo Wanu Wabanja Kukhala Wachimwemwe. Ndatsekeramo K8.00.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena