Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g88 2/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1988
Galamukani!—1988
g88 2/8 tsamba 2

Tsamba 2

Makolo mamiliyoni angapo kuzungulira dziko lonse ataikiridwapo mwana. Matenda, njala, nkhondo, kuphedwa, kudzipha, ngozi, imfa ya mwangozi, kupita padera, kubala mwana wakufa—mosasamala kanthu ndi chomwe chingakhala chochititsa, kholo nthaŵi zonse limakhala ndi chisoni.

Mosasamala kanthu za msinkhu wa mwana, kuŵaŵa nthaŵi zonse kumakhalapo. Kodi chisonicho chingapiriridwe motani? Kodi ndimotani mmene moyo ungapitirizirebe? Kodi chisonyezero chathu patsambali cha banja likulandiranso mwana wawo kuchokera kwa akufa chiri kokha loto, kapena kodi icho posachedwapa chidzakhala chenicheni?

Nkhani zowona zotsatirazi za anthu omwe apulumuka chisoni chowopsya chochititsidwa ndi kutaikiridwa kwa mwana zidzayankha ena a mafunso ameneŵa. Kaamba ka zotulukapo mu chimodzi ndi chimodzi cha izo, chonde ŵerengani nkhanizi za chisoni. Tikhulupirira kuti mudzapeza chitonthozo ndi chiyembekezo kuchokera mu izo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena