Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g88 1/8 tsamba 32
  • “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
  • Galamukani!—1988
Galamukani!—1988
g88 1/8 tsamba 32

“Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”

Liri pamwambali liri lonjezo lochokera kwa Mulungu lomwe linatengedwa monga mutu wa kabroshuwa katsopano. Kodi lonjezolo limatanthauzanji kaamba ka ife? Kodi lidzakwaniritsidwa motani, ndipo liti?

Pezani mwakuŵerenga chofalitsidwa chabwino kwambiri, cha masamba 32. Chidzatumizidwa kwa inu pamodzi ndi mabroshuwa a Boma Limene Lidzabweretsa Paradaiso ndi Sangalalani ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!, kokha pa K7.20.

Chonde nditumizireni, mutalipiriratu positi, timabroshuwa titatu “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano,” Boma Limene Lidzabweretsa Paradaiso, ndi Sangalalani ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha! Ndatsekeramo K7.20.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena