Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g88 3/8 tsamba 32
  • Nchiyani Chimene Mboni za Yehova Zimakhulupirira?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nchiyani Chimene Mboni za Yehova Zimakhulupirira?
  • Galamukani!—1988
Galamukani!—1988
g88 3/8 tsamba 32

Nchiyani Chimene Mboni za Yehova Zimakhulupirira?

Atsogoleri a m’midzi mu Roma wa zana loyamba anauza mtumwi Wachikristu Paulo kuti: “Tikufuna kumva zimene mukhulupirira, pakuti chinthu chokha chimene tidziŵa ponena za Akristu amenewa chiri chakuti awanenera ponse ponse!” (Machitidwe 28:22, The Living Bible) Anthu amenewo anafuna kumva kuchokera ku magwero m’malo mwa osuliza akunja okha.

Lerolino, Mboni za Yehova zimaneneredwa moipa kaŵirikaŵiri, ndipo chikakhala kulakwa kuyembekezera kuphunzira chowonadi ponena za iwo kuchokera ku magwero osuliza. Chotero tiri osangalatsidwa kugaŵira mabroshuwa atatu a masamba 32 amene amalongosola zikhulupiriro za Mboni za Yehova, otchedwa Jehovah’s Witnesses in the Twentieth Century, School and Jehovah’s Witnesses, ndi Mboni za Yehova—Zikuchita Chifuniro cha Mulungu Mogwirizana pa Dziko Lonse Lapansi, kokha pa K7.20.

Chonde tumizani, mutalipiriratu positi, mabroshuwa atatu Jehovah’s Witnesses in the Twentieth Century, School and Jehovah’s Witnesses, ndi Mboni za Yehova—Zikuchita Chifuno cha Mulungu Mogwirizana pa Dziko Lonse Lapansi. Ndatsekeramo K7.20.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena