Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g89 8/8 tsamba 32
  • Mmene Ukwati Uwu Unapulumutsidwira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mmene Ukwati Uwu Unapulumutsidwira
  • Galamukani!—1989
Galamukani!—1989
g89 8/8 tsamba 32

Mmene Ukwati Uwu Unapulumutsidwira

“Kugwiritsiridwa ntchito kwa uphungu wa m’bukhu lakuti Kupangitsa Moyo Wanu wa Banja Kukhala Wachimwemwe kunapulumutsa ukwati wanga,” analemba tero muŵerengi woyamikira wa ku South Africa. “Mutu 5, ‘Mkazi Amene Ali Wokondedwa Kwambiri,’ unatsegula maso anga. Sindinaganizire konse m’maloto anga oipa kuti ndingachititse mavuto ambiri chotero popanda kulingalira. Ndikuyamikirani kwabasi. Ukwati wanga unali m’mbali za mafunde kwenikweni a m’nyanja, ndipo tsopano, pambuyo pa miyezi ingapo, wabwereranso pa doko la bata lachimwemwe.”

Ngati inu mukukhumba thandizo m’kupangitsa ukwati wanu kukhala wachimwemwe koposapo, mungapindule kuchokera m’bukhu limeneli. Landirani kope mwa kudzaza ndi kutumiza kapepalaka.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena