Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g90 3/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1990
Galamukani!—1990
g90 3/8 tsamba 2

Tsamba 2

Kwa zaka mazana ambiri Spanya ndi Chikatolika zawonekera kukhala zosalekanitsika mofanana ndi Mariya ndi khandalo. Kucheza kwachipambano kwa papa ku Spanya mu 1982, mkumene mamiliyoni ambiri analandira John Paul II ndi mawu akuti Totus tuus (Zonse nzanu), anatsimikizira poyera kudzipereka kwa dzikolo ku chipembedzo chake cha makolo.

Koma chisangalalocho chitazirala, kutsutsana kosalekeza kunakhalapobe—kwina nkwakalekale, kwina nkoyambira m’nthaŵi yathu. Nkhani zotsatirapozo zidzasanthula kwina kwa kutsutsana kumeneku limodzi ndi zochititsa zake ndi matanthauzo awo kwa tchalitchi Chachispanya champhamvuyonse panthaŵi ina.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Agencia EFE

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena