Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g90 2/8 tsamba 32
  • Kodi Baibulo Liri Kokha Bukhu Lina?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Baibulo Liri Kokha Bukhu Lina?
  • Galamukani!—1990
Galamukani!—1990
g90 2/8 tsamba 32

Kodi Baibulo Liri Kokha Bukhu Lina?

Ngati nditero, nchifukwa ninji ilo lawukiridwa mowopsya chotero m’mbiri yonse? Kodi mungalikhulupirire Baibulo? Kodi zozizwitsa zolembedwamo zinachitikadi? Kodi sayansi yatsimikizira Baibulo kukhala lolakwa?

Mayankho a mafunso ameneŵa ngofunika kwambiri, popeza kuti Baibulo limaneneratu za chiwonongeko cha dziko chomayandikira ndipo limapereka njira yopulumukira. Bukhu lakuti The Bible—God’s Word or Man’s? lidzakupatsani mayankho okhutiritsa. Tumizani K20 yokha kaamba ka kope lanu laumwini.

Chonde tumizani, mutalipiriratu positi, bukhu lachikuto cholimba, lamasamba 192 lakuti The Bible—God’s Word or Man’s? Ndatsekeramo K20(Zambia).

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena