Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g90 8/8 tsamba 32
  • Kodi Mulungu Amaloleranji Mavuto?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mulungu Amaloleranji Mavuto?
  • Galamukani!—1990
Galamukani!—1990
g90 8/8 tsamba 32

Kodi Mulungu Amaloleranji Mavuto?

Mbiri yoipa iri chochitika chenicheni m’moyo, koma kodi nchifukwa ninji iri yofala motero? Kodi nchifukwa ninji pali mavuto ochuluka motero? Kodi kukhalapo kwake kungagwirizanitsidwe motani ndi kukhulupirira Mulungu wachikondi? Kodi mavuto adzatha konse?

Mayankho amafunso ameneŵa ndi ena ofunika kwambiri akupezeka m’Baibulo. Mayankhowo amaphatikizapo inu ndi banja lanu. Amaphatikizapo chimwemwe chanu. Buku lakuti Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha m’Paradaiso pa Dziko Lapansi limapereka chiyembekezo mwakukusonyezani mayankho a Baibulo.

Masamba 256 a bukulo, aukulu wa magazini ano, adzaza ndi zithunzithunzi zophunzitsa zoposa 150, zambiri nzamawonekedwe okongola. Ngati mungafune kulandira kope, chonde lembani ndikutumiza kapepala kali pansipa.

[Mawu a Chithunzi patsamba 32]

U.S. Army

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena