Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g90 9/8 tsamba 32
  • “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”
  • Galamukani!—1990
Galamukani!—1990
g90 9/8 tsamba 32

“Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano”

Lomwe liri pamwambalo ndi lonjezo lochokera kwa Mulungu lomwe latengedwa kukhala mutu wa broshuwa yokongola. Kodi lonjezolo likutanthauzanji kwa inu? Kodi lidzakwaniritsidwa motani, ndipo liti?

Inu mungadziwonere nokha mwakuŵerenga bukhu lokongolali lamasamba 32. Ngati mukufuna kulandira kope, chonde dzazani ndi kutumiza kapepala komwe kali pansipa.

Ndingakonde kulandira broshuwa yamasamba 32 yakuti “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano” (Kunja kwa Zambia, lemberani nthambi ya Watch Tower ya kumaloko kaamba ka chidziŵitso. Onani tsamba 4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena