Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g90 12/8 tsamba 32
  • Zisonyezero za Volyumu 34 ya Galamukani!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Volyumu 34 ya Galamukani!
  • Galamukani!—1990
  • Timitu
  • ACHICHEPERE AKUFUNSA KUTI
  • CHIPEMBEDZO
  • CHUMA NDI NTCHITO YOLEMBEDWA
  • LINGALIRO LA BAIBULO
  • MAIKO NDI ANTHU
  • MAUNANSI A ANTHU
  • MBONI ZA YEHOVA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • NYAMA NDI ZOMERA
  • ULAMULIRO WA ANTHU UYESEDWA
  • UMOYO NDI MANKHWALA
  • ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MAKHALIDWE
Galamukani!—1990
g90 12/8 tsamba 32

Zisonyezero za Volyumu 34 ya Galamukani!

ACHICHEPERE AKUFUNSA KUTI

Amai ndi Atate Ali Osaphunzira—Kodi Ndingawalemekeze Bwanji? 1/8

Kholo Lomwe Linachoka Panyumba, 11/8

Kodi Nchifukwa Ninji Izi Zikuchitika ku Thupi Langa? 2/8

Kodi Nchiyani Chikuchitika ku Thupi Langa? 2/8

Kodi Ndibatizidwe? 4/8

Kodi Ndimotani Mmene Ndingathetsere Kusungulumwa Kwanga? 1/8

Kodi Ndine Wokonzeka Kubatizidwa? 4/8

Kodi Ndingasankhe Motani Kanema Yabwino? 8/8

Kodi Ndiyenera Kudziperekeranji Kaamba ka Ena? 6/8

Kodi Nkuliphunziriranji Baibulo? 10/8

Kodi Ziri Nkanthu Akanema Amene Ndimawonerera? 8/8

Kudzikometsera, 6/8

Kukhala ndi Kholo Limodzi, 7/8

Kukhala ndi Pakati kwa Achichepere, 5/8

Kupanga Kupita Patsogolo Kwauzimu, 10/8

Kupeŵa Matsenga, 3/8

Makolo Amandichititsa Manyazi, 3/8

Makolo Anga Akulekana—Kodi Ndichitenji? 9/8, 11/8

Masitayelo ndi Mipikisano ya Kukongola, 1/8

Nchifukwa Ninji Kudzimva Wopanda Chisungiko? 5/8

Ntchito Yapambuyo Poŵeruka Kusukulu, 12/8

Zopakapaka, 7/8

CHIPEMBEDZO

Chifukwa Chimene Mulungu Analola Kuvutika, 10/8

Kukongola Kwamuyaya kwa Chipembedzo Chowona, 1/8

Kulekana Kwatsopano, 7/8

Mafunso Omwe Amafunikira Kuyankhidwa, 10/8

Nchifukwa Ninji Pali “Kuda Nkhaŵa Kwakukulu,” 7/8

Nchifukwa Ninji Pali Kugaŵanikana? 7/8

Tchalitchi cha Chikatolika mu Spanya—Kodi Nchifukwa Ninji Vutolo? 3/8

Tchalitchi cha Chikatolika mu Spanya—Kugwiritsira Ntchito Ulamuliro Molakwa, 3/8

Tchalitchi cha Chikatolika mu Spanya—Ulamuliro ndi Mwaŵi, 3/8

Tchalitchi cha Chikatolika mu Spanya—Zitsutsano, 3/8

Ufulu, 10/8

CHUMA NDI NTCHITO YOLEMBEDWA

Ngongole! Kuloŵamo—Kutulukamo, 2/8

LINGALIRO LA BAIBULO

Angelo, 3/8

Ayuda Anthu Osankhidwa a Mulungu? 7/8

Hanukkah—Kodi Ndiyo “Krisimasi” Yachiyuda? 12/8

Kodi Ndiliti Pamene Moyo wa Munthu Umayambika? 10/8

Kodi Sayansi Yapangitsa Baibulo Kukhala Lachikale? 8/8

Korona, 6/8

Kudzipha—Kodi Pali Chiukiriro? 9/8

Mankhwala Ogodomalitsa Ngosangulutsira—Chifukwa Ninji Ayi? 11/8

Mdyerekezi Alikodi? 1/8

Pemphero m’Maseŵera, 5/8

Tchimo Loyambirira, 4/8

MAIKO NDI ANTHU

Thanthwe la Gibraltar, 1/8

Ulendo wa Pamtsinje wa Chobe (South Africa), 8/8

MAUNANSI A ANTHU

Anthu a Fuko Lina—Kodi Mumaŵalingalira Motani? 12/8

Apongozi—Kodi Chimachititsa Vutolo Nchiyani? 3/8

Apongozi—Kusangalala Unansi Wabwino, 3/8

Apongozi—Mkangano Wakalekale, 3/8

Kupyolera m’Maso Amwana, 2/8

Makhalidwe Abwino Kubwereranso? 6/8

Mapindu a Makhalidwe Abwino Amene Amabweretsa Chimwemwe, 6/8

Zomwe Timadziŵa Ponena za Fuko, 12/8

MBONI ZA YEHOVA

Adokotala ndi Mboni Zodwala, 12/8

Chivomerezo cha Oŵerenga Bukhu la Young People Ask, 9/8

Ubale Wapadziko Ngotsimikizirika, 12/8

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Achichepere Amakono—Akumana Ndi Zitokoso za m’ma 1990, 9/8

Achichepere Amakono—Chithunzi cha Padziko Lonse, 9/8

Achichepere Amakono—Zitokoso Zimene Amakumana Nazo, 9/8

‘Chizoloŵezi Choipachi Chakusuta Fodya,’ 8/8

Choipitsitsa Kuposa AIDS, 2/8

Dziko Latsopano Lopanda Mavuto, 10/8

Khutu—Wolankhulira Wamkulu, 2/8

Kodi Ndimphatso ya Moyo Kapena Mpsopsono wa Imfa? 11/8

Kodi Nthaŵi Zonse Mumachedwa? 1/8

Mabuku Aulere, 9/8

Madzi Amtengo Wapatali Kwenikweni m’Dziko, 11/8

Maphindu Osintha ndi Kupita kwa Mbiri, 6/8

Mmene Mungachitire Zambiri mu Nthaŵi Yochepa, 6/8

Moyo Kunja kwa Dziko Lapansi—Kodi Kuli Aliyense Kunja Kumeneko? 4/8

Zamoyo Zakuthambo—Kodi Ziri Kuti? 4/8

Zamoyo Zakuthambo—Kupeza Yankho, 4/8

Zamoyo Zakuthambo—Loto Lakalekale, 4/8

NYAMA NDI ZOMERA

Kodi Nchiyani Chimene Chinachitika kwa Madinosaur? 2/8

Kodi Ndani Amene Akupha Nkhalango Zamvula? 4/8

Kodi Nkhalango Ziri ndi Mtsogolo? 4/8

Kodi Nkusungiranji Nkhalango Zamvula? 4/8

Kufufuza Nyama—Dalitso Kapena Temberero? 7/8

Kufufuza Nyama—Kawonedwe Kolinganizika, 7/8

Kufufuza Nyama—Zivomerezo Zachiwawa, 7/8

Kupeza ‘Zokwawa Zazikulu’ Zakale, 2/8

Mawonekedwe ndi Maukulu Osiyana a Madinosaur, 2/8

“Pitani ku Nyerere,” 6/8

Walrus ndi Malonda a Mankhwala Ogodomalitsa, 2/8

Wosangalatsa Wofiirayo ndi Nyimbo Yosangalatsa, 3/8

ULAMULIRO WA ANTHU UYESEDWA

“Anthufe,” 10/8

‘Boma Lolamulidwa ndi Abwino,’ 9/8

Kufunafuna Utopia kwa Ndale Zadziko, 11/8

Kulamulira kwa Munthu Kufikira Mapeto Ake, 12/8

Mafumu, Amakwera ndi Kugwa, Mofanana ndi Nyenyezi, 9/8

Malaya Akuda ndi Maswastika, 11/8

Mphamvu Zopanda Malire—Dalitso Kapena Temberero? 10/8

Nsanganizo Wandale Zadziko wa Chitsulo ndi Dongo, 11/8

Ulamuliro wa Anthu Uyesedwa Pamiyeso— Chifukwa Ninji? 8/8

UMOYO NDI MANKHWALA

Chikhulupiriro Chinandithandiza Kuyang’anizana Ndi Opareshoni ya Ubongo, 5/8

Kodi Kugulitsa Mwazi Kuli Bizinesi Yaikulu, 11/8

Kodi Kuthiridwa Mwazi Ndiko Mfungulo Yopulumukira? 11/8

Kodi Tingakhale kwa Utali Wotani? 5/8

Kufunafuna Moyo Wautali, 5/8

Kukhala ndi Khunyu, 7/8

Makanda, Mwazi, ndi AIDS, 7/8

Minkhole Yopepuka ya Fodya, 10/8

Mtengo wa Kusawona Mtima (Nkhani Yamwazi), 10/8

Mtundu Woipitsitsa wa Kuipsya Mwana (Kusuta), 1/8

Pamene AIDS Siirinso Chiwopsezo, 3/8

“Sindidzayendanso,” 9/8

ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MAKHALIDWE

Achichepere—Zitokoso za m’ma 1990, 9/8

Ana Opanda Kokhala—Kodi Nchifukwa Ninji Kuli Kovuta Kuthandiza? 1/8

Ana Opanda Kokhala—Kodi Ndani Ali ndi Liŵongo? 1/8

Ana Opanda Kokhala—Kodi Pali Yankho? 1/8

Dziko Laudongo—Tikulifunadi, 5/8

Kodi Tifunikiradi Boma? 8/8

Kuipitsa—Kodi Ndani Akukuchititsa? 5/8

Kumwerekera ndi Crack—Kodi Pali Njira Yokuthetsera, 8/8

Kumwerekera ndi Crack—Mliri Wake wa Chiwawa, 8/8

Kumwerekera ndi Crack—Tsoka kwa Ana Osabadwa, 8/8

Kutembenuzira Chisamaliro pa Boma, 8/8

Malo Otizinga Omanyonyotsoka, 2/8

Mapeto a Kuipitsa Ali Pafupi, 5/8

Ma 1990—Zaka Khumi Zosatsimikizirika, 8/8

Mfuti—Dziko Lopanda Izo, 6/8

Mfuti—Njira ya Imfa, 6/8

Mfuti—Njira ya Moyo, 6/8

Mfuti—Sizaamuna Okha, 6/8

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena