Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g91 3/8 tsamba 32
  • Chochitika Chimene Simuyenera Kuphonya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chochitika Chimene Simuyenera Kuphonya
  • Galamukani!—1991
Galamukani!—1991
g91 3/8 tsamba 32

Chochitika Chimene Simuyenera Kuphonya

‘Chitani ichi chikumbukiro changa.’ Mawu ameneŵa a Ambuye wathu Yesu Kristu, opezeka pa Luka 22:19, ananenedwa panthaŵi imene iye anakhazikitsa chikumbutso cha imfa yake. Imfa ya Yesu ndiyo inatsegulira anthu chiyembekezo chakupeza moyo wosatha m’mikhalidwe ya Paradaiso. Chotero imfa yake ndichinthu chimene tiyenera kukumbukira. Kodi mudzachita chikumbutso chake chaka chino?

Chonde landirani chiitanochi chochokera kwa Mboni za Yehova chakuti mugwirizane nawo m’kukumbukira chochitika chofunika kwambiri chimenechi. Chikumbukiro chimenechi chidzachitika dzuŵa litaloŵa padeti lolingana ndi Nisani 14 ya kalenda ya Baibulo yozikidwa pa mayendedwe a mwezi. Ikani chizindikiro pa detilo pakalenda yanu kuti musaiŵale. Ilo ndi Loŵeruka, March 30, 1991. Yemwe akukupatsani chiitanochi angakuuzeni malo okumanirako enieniwo ndi nthaŵi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena