Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g91 4/8 tsamba 32
  • Uthenga wa Lerolino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Uthenga wa Lerolino
  • Galamukani!—1991
Galamukani!—1991
g91 4/8 tsamba 32

Uthenga wa Lerolino

Nsanja ya Olonda iri ndi uthenga wotero, monga momwe ananenera woŵerenga wina yemwe posachedwapa anapempha sabusikripishoni. Mkaziyo analemba kuti: “Ndakhala ndikuwêrenga magazini anu ndichikondwerero chachikulu. Ndinali ndi mwaŵi woŵerenga male-mba m’nkhani zosiyanasiyana mkati mwa nthaŵi yanga yopuma.

“Ndimazizwa nthaŵi zonse ndi uthenga wa magazini anu ponena za nyuzi zamakono. Palibe kugogomezera kumene kungachitidwe kosonyeza kufunika kwa mabuku anu kaamba ka kumvetsetsa kwabwinopo kwa Baibulo. Magazini anu ndiwo anandichititsa kutenga Baibulo lodzala ndi fumbi ndi kufufuza m’Bukhulo loposa mabuku onse. Ndimayembekezera mwachidwi kope lirilonse.”

Kodi mungakonde kuti Nsanja ya Olonda itumizidwe kunyumba kwanu? Ngati nditero, chonde dzazani ndi kutumiza kapepala kotsatiraka.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena