Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g92 1/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1992
  • Timitu
  • Nkhaŵa za Ndalama—Kodi Zidzathadi? 3-8
  • Kukwatirana Kapena Kukhalira Pamodzi—Kodi Choyenera Nchiti? 30
Galamukani!—1992
g92 1/8 tsamba 2

Tsamba 2

Nkhaŵa za Ndalama—Kodi Zidzathadi? 3-8

“Ndalama nzofunika,” analemba tero Galbraith, katswiri wa zachuma. “Zimalingana ndi chikondi monga magwero aakulu koposa a chimwemwe cha munthu. Ndipo zimalingana ndi imfa monga magwero aakulu koposa a nkhaŵa yake.” Dongosolo lazachuma lamakono limadzetsa maupandu, nkhaŵa ndi zikhumbo. Nkhani zathu zoyambirira nzimene zipanga Gawo 1 m’mpambo wa magawo 6 m’miyezi itatu yotsatira amene adzafotokoza mbiri ya dongosolo lamalonda ndi ntchito ya ndalama m’chitukuko cha anthu.

Kukwatirana Kapena Kukhalira Pamodzi—Kodi Choyenera Nchiti? 30

Mamiliyoni ambiri lerolino amasankha kukhalira pamodzi popanda mapindu a ukwati. Kodi lingaliro la Baibulo pa nkhaniyi nlotani?

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

With kind permission of the Kunsthistorisches Museum, Vienna

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena