Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g95 4/8 tsamba 32
  • Deti Limene Simuyenera Kuiŵala

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Deti Limene Simuyenera Kuiŵala
  • Galamukani!—1995
Galamukani!—1995
g95 4/8 tsamba 32

Deti Limene Simuyenera Kuiŵala

Madzulowo Yesu asanamwalire, anagaŵana mtanda wa mkate wopanda chotupitsa ndi chikho cha vinyo ndi atumwi ake nati: “Chitani ichi chikumbukiro changa.”—Luka 22:19.

Chaka chino chochitikacho chidzakhalako pa Lachisanu April 14 dzuŵa litaloŵa. Chifukwa cha kumvera lamulo la Yesu, mamiliyoni a Mboni za Yehova ndi anthu okondwerera padziko lonse adzasonkhana usiku wapadera umenewu kuchitanso Chikumbutso chimenechi m’njira imene Yesu analangiza. Mukuitanidwa mwachikondi kudzasonkhana nafe. Chonde funsani Mboni za Yehova za kwanuko ponena za nthaŵi yeniyeni ndi malo osonkhanira.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena