Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g95 5/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1995
  • Timitu
  • Kodi Ano Ndiwo Masiku Otsiriza? 3-11
  • Zaka Zoposa 40 Pansi pa Chiletso cha Komyunizimu 19
Galamukani!—1995
g95 5/8 tsamba 2

Tsamba 2

Kodi Ano Ndiwo Masiku Otsiriza? 3-11

Popeza kuti Baibulo lili ngati mapu a msewu, kodi ilo limasonyeza pamene tili? Kodi tikukhala m’masiku otsiriza? Ngati ndi choncho, kodi nchiyani chimene chili patsogolopa? Kodi tiyenera kuchitanji?

Zaka Zoposa 40 Pansi pa Chiletso cha Komyunizimu 19

Mboni za Yehova zambiri ku Eastern Europe zinakhala ndi moyo pansi pa chiletso kwa zaka zoposa 40. Ŵerengani zokumana nazo zokondweretsa za Mboni ina Yachitcheki.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

CHIKUTO: Kuzungulira kuyambira kulamanja kumka kulamanzere, Majeti ankhondo: Chithunzi cha USAF; Laŵi la moto: Tina Gerson/Los Angeles Daily News; Jeti yoponya mabomba: Mwachilolezo cha Unduna wa Zachitetezo, London; Msilikali: Chithunzi cha U.S. National Archives (onaninso masamba 2, 7); TSAMBA LACHIŴIRI: Kuphulika kwa bomba la nyukliya: Chithunzi cha U.S. National Archives (onaninso tsamba 7); Mwana wanjala: Mark Peters/Sipa Press (onaninso tsamba 8)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena