Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g99 9/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1999
  • Timitu
  • Kodi Kuopa Nyukiliya Kwatha? 3-11
  • Kutumikira Mulungu Poyang’anizana ndi Imfa 18
Galamukani!—1999
g99 9/8 tsamba 2

Tsamba 2

Kodi Kuopa Nyukiliya Kwatha? 3-11

Pamene mkangano wapakati pa dziko la United States ndi Russia unatha, anthu ambiri anasangalala kuti mtundu wa anthu sudzaopsedwanso ndi nkhondo ya nyukiliya. Komabe nkhani zotsatirazi zikulongosola zina mwa zifukwa zimene tinganenere kuti zida za nyukiliya zidakali kuopseza anthu kwambiri kuposa mmene anthu ambiri amaganizira.

Kutumikira Mulungu Poyang’anizana ndi Imfa 18

Kwa zaka zambiri anapirira kuzunzidwa ndiponso anatsekeredwa m’ndende ndi kutumizidwa ku ukaidi. Ŵerengani nkhani yolimbikitsa ya munthu wa ku Afirika ameneyu.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Bomba lophulika lili pachikutopo: UNITED NATIONS/PHOTO BY SYGMA

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena