Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g04 12/8 tsamba 32
  • Mlozera Nkhani wa Voliyumu 85 ya Galamukani!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mlozera Nkhani wa Voliyumu 85 ya Galamukani!
  • Galamukani!—2004
  • Timitu
  • ACHINYAMATA AKUFUNSA
  • CHIPEMBEDZO
  • CHUMA NDI NTCHITO
  • MAUNANSI A ANTHU
  • MAYIKO NDI ANTHU
  • MBONI ZA YEHOVA
  • NKHANI ZA MOYO WA ANTHU
  • SAYANSI
  • UMOYO NDI MANKHWALA
  • ZIMENE BAIBULO LIMANENA
  • ZINYAMA NDI ZOMERA
  • ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE
  • ZOSIYANASIYANA
Galamukani!—2004
g04 12/8 tsamba 32

Mlozera Nkhani wa Voliyumu 85 ya Galamukani!

ACHINYAMATA AKUFUNSA

Kugonana kwa pa Telefoni, 3/8

Kugonana Ndisanalowe M’banja, 8/8, 9/8

Kumwa Mowa Wambiri Nthawi Imodzi Kuli ndi Vuto Lanji? 10/8

Kupeza Nthawi Yochita Homuweki, 2/8

Malo Ovinira, 5/8

N’chifukwa Chiyani Chibwenzi Changa Chimandizunza Chonchi? 6/8

N’chifukwa Chiyani Mulungu Amalola Kuti Tizivutika? 4/8

Ndingamuuze Bwanji Kuti Ndikumufuna? 11/8

Ndingatani Kuti Chibwenzi Changa Chisiye Kundizunza? 7/8

Ndingathe Bwanji Kukamba Nkhani Bwino Pagulu? 1/8

Ndingachite Chiyani Ndikalephera? 12/8

CHIPEMBEDZO

Kudziwa Dzina la Mulungu, 2/8

Mose Anali Munthu Weniweni Kapena Wongopeka? 4/8

CHUMA NDI NTCHITO

Kuvutitsidwa kuntchito, 5/8

MAUNANSI A ANTHU

Achinyamata Akamakula, 7/8

Atate Abwino, 9/8

Kulimbikitsa Ana Kuti Azikonda Kuphunzira, 8/8

Kusungulumwa, 6/8

Kupeza Anzanu Enieni, 12/8

Kuwerengera Ana, 11/8

Sukulu Yamkaka Yopanda Zoseweretsa, 10/8

Sungani Nthawi! 4/8

Zaka Zoyambirira za Moyo wa Mwana, 11/8

Zimene Ana Amafunikira Kwa Makolo, 1/8

MAYIKO NDI ANTHU

Anapulumuka Madzi Atasefukira! (Switzerland), 4/8

Mathithi (Zambia), 3/8

Msika wa Nsomba Waukulu Kwambiri Padziko Lonse (Japan), 2/8

Namaqualand (South Africa), 2/8

MBONI ZA YEHOVA

Achinyamata Amene Sachita Manyazi Kulankhula, 9/8

“Aliyense Ayenera Kuwerenga Buku Limeneli” (Mphunzitsi), 12/8

Banja Liyesedwa Chikhulupiriro, 5/8

Chikhulupiriro Chiyesedwa (Richmond Sixteen), 3/8

Khoti la ku Ulaya Linalemekeza Ufulu wa Mayi (France), 12/8

Msamariya Wachifundo Wamakono, 8/8

Zosuta Fodya Ine Ayi! (ndakatulo ya mtsikana), 5/8

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

Chinthu Chabwino Kuposa Kutchuka (C. Sinutko), 9/8

Ndinaphunzitsidwa Kukonda Mulungu Kuyambira Ndili Mwana (A. Melnik), 11/8

“Yehova, Mwandipeza!” (N. Lenz), 10/8

SAYANSI

Kuyeza Dziko Lapansi ndi Ndodo, 7/8

Sayansi Ingakuthandizeni Kudziwa Mulungu? 7/8

UMOYO NDI MANKHWALA

Banja Liyesedwa Chikhulupiriro (matenda a zilonda za m’mimba), 5/8

Chimfine Chobwera Mukakhala Pafupi ndi Mungu, 6/8

Kodi Edzi Idzatha Liti? 12/8

Kugona Tulo Tosakwanira, 2/8

Kunenepa Kwambiri, 11/8

Kusabereka, 10/8

Mankhwala Ochokera ku Zitsamba, 1/8

Matenda a Maganizo 1/8

Matenda a Misala, 12/8

Matenda Osintha Mtundu wa Khungu 10/8

Ngati Mwana Wakhanda Sasiya Kulira, 5/8

Nkhawa ya Maonekedwe Ikasanduka Matenda, 8/8

Nkhondo Yolimbana ndi Matenda, 6/8

Timafuniranji Chiyembekezo? 5/8

ZIMENE BAIBULO LIMANENA

Anthu Okalamba Tiyenera Kuwachitira Zinthu Motani? 10/8

Khalidwe Limayendera Gulu la Magazi? 2/8

Kodi Kusudzulana N’kuthetsadi Mavuto? 12/8

Kuda Nkhawa N’kupanda Chikhulupiriro? 6/8

Kulera Ana M’maleredwe a Mulungu, 11/8

Kumwa Mowa Mwauchidakwa N’koipadi? 3/8

Mulungu Amawaganiziradi Ana? 8/8

Mutu wa Banja, 7/8

N’chifukwa Chiyani Ukwati Tiyenera Kuuona Kuti N’ngopatulika? 5/8

N’zotheka Kusiya Zizolowezi Zoipa? 4/8

Zokambirana za Mayiko Zidzabweretsa Mtendere Padziko Lonse? 1/8

N’zotheka Kusiya Zizolowezi Zoipa? 4/8

Zokambirana za Mayiko Zidzabweretsa Mtendere Padziko Lonse? 1/8

ZINYAMA NDI ZOMERA

Chomera Chopirira Modabwitsa (welwitschia), 3/8

Lavenda, 7/8

Mphaka Amene Ali Pangozi Kwambiri (lynx wa ku Spain), 8/1

Ziweto, 3/8

Zomera N’zothandiza Popanga Mankhwala, 1/8

ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE

Kudziteteza ku Anthu Oba Mwachinyengo, 8/8

Kusintha Zinthu, 4/8

Kutenga Mimba Ali Ana, 10/8

Nkhondo ya Nyukiliya Akuiopabe? 3/8

Tsankho, 9/8

ZOSIYANASIYANA

Chiwerengero cha Anthu, M’Baibulo, ndi M’tsogolo, 5/8

Chiyembekezo, 5/8

Kukhalabe Osangalala Ngakhale M’mavuto, 1/8

Kukonda Kuphunzira, 8/8

Matayala, 6/8

Mowa, 7/8

Zoseweretsa Ana Zabwino Kwambiri, 8/8

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena