Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 12/06 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2006
  • Nkhani Yofanana
  • Calypso Nyimbo Zamakolo za ku Trinidad
    Galamukani!—2006
  • Muzisankha Zinthu Mwanzeru pa Nkhani ya Mowa
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Kodi Kumwa Mowa N’kulakwa?
    Galamukani!—2006
  • Kuchokera kwa Owerenga
    Galamukani!—2008
Onani Zambiri
Galamukani!—2006
g 12/06 tsamba 1-2

Zamkatimu

December 2006

Kodi Yesu Anali Ndani?

Kodi anthu olemba mbiri amati Yesu ndi wofunika motani? N’chifukwa chiyani iye ali wosiyana ndi anthu ena onse? Nanga n’chifukwa chiyani zimenezo ziyenera kukhala zofunika kwa ife?

3 Munthu Woposa Onse Amene Anakhalapo

4 Chifukwa Chake Iye Ali Wofunika Kwambiri

7 Moyo Umene Adzabweretse

10 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

N’chifukwa Chiyani Amandiikira Malamulo Ambirimbiri?

16 “Unabadwa kwa Makolo Oyera Kuposa Onse”

20 “Kodi Mumakondwerera Tsiku la Agogo Aakazi?”

21 Anakonda Zimene Anaphunzira

24 Calypso Nyimbo Zamakolo za ku Trinidad

26 Kodi Tikanatani Pakadapanda Abulu?

28 Kuchokera kwa Owerenga

29 Zochitika Padzikoli

30 Mlozera Nkhani wa Magazini A Galamukani! a 2006

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Mphatso Yamtengo Wapatali

Ndinali Mwana Wolowerera 13

Werengani za mnyamata amene anapandukira makolo ake oopa Mulungu ndiponso zimene zinam’chititsa kuti asinthe moyo wake n’kubwerera.

Kodi Kumwa Mowa N’kulakwa? 18

Baibulo limanena za mavuto amene angabwere chifukwa cha mowa. Choncho, kodi kumwa mowa n’koyenera?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena