Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 12/09 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2009
  • Nkhani Yofanana
  • Mawu Oyamba
    Galamukani!—2021
  • Nthenga za Kadzidzi
    Galamukani!—2009
  • Kodi Mungathetse Bwanji Njala Yanu Yauzimu?
    Galamukani!—2009
  • Kodi Zinthu Zinachita Kulengedwa Kapena Zinangokhalapo Zokha?
    Galamukani!—2009
Onani Zambiri
Galamukani!—2009
g 12/09 tsamba 1-2

Zamkatimu

December 2009

N’chifukwa Chiyani Mulungu Analenga Zonsezi?

Asayansi ambiri sagwirizana ndi maganizo akuti pali winawake amene anapanga dzikoli ndiponso kuti anali nalo cholinga. Komabe, pali mfundo zomveka zosonyeza kuti pali winawake amene anapanga anthu ndiponso dzikoli ndipo anali nalo cholinga.

3 Chilengedwe N’chogometsa

4 Kodi Zinthu Zinachita Kulengedwa Kapena Zinangokhalapo Zokha?

9 N’chifukwa Chiyani Tili ndi Moyo?

11 Kodi Nyenyezi Imene Inatsogolera “Anzeru a Kum’mawa” Inali Yotani?

14 Zochitika Padzikoli

15 Nyama Zikuluzikulu za M’nyanja

18 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndingatani Kuti Ndizilankhula Momasuka ndi Makolo Anga?

22 Ubwino Wosonyezana Chikondi

23 Panagona Luso!

Nthenga za Kadzidzi

28 Samalani ndi Poizoni

30 Mlozera Nkhani wa Magazini a Galamukani! a 2009

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Analimba Mtima Kufotokoza Zimene Amakhulupirira

Kodi Mungathetse Bwanji Njala Yanu Yauzimu? 12

Ena amaganiza kuti angathetse njala yawo yauzimu pochita miyambo yosiyanasiyana yachipembedzo kapena yachikhalidwe. Kodi njira iliyonse yothetsera njala yanu yauzimu ndi yovomerezeka? Werengani nkhaniyi kuti mumve zimene Baibulo limanena.

Chimene Chinandichititsa Kusiya Kukonda Nkhondo 24

Werengani nkhani yochititsa chidwi ya munthu wina amene ankakonda nkhondo kwambiri koma kenako anasiya atapeza zochita zina zabwino.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena