Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • fu tsamba 1-2
  • Mutu wa Kabuku Kano/Tsamba la Ofalitsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mutu wa Kabuku Kano/Tsamba la Ofalitsa
  • M’tsogolo Mosungika—M’mene Mungamupezere
M’tsogolo Mosungika—M’mene Mungamupezere
fu tsamba 1-2

Mutu wa Kabuku Kano/Tsamba la Ofalitsa

M’tsogolo Mosungika—M’mene Mungamupezere

Ngati mukufuna moyo m’mikhalidwe yosungika, mudzapeza zimene zalongosoledwa m’kabukhu’ka kukhala zolimbikitsa kwambiri. Komabe, kuphatikiza pakukawerenga kwanu, tikukhulupirira kuti mudzafuna kukambitsirana zamkati mwake ndi munthu wina amene amazindikira bwino Baibulo, chifukwa chakuti zinthu zimenezi zimakhudza kwambiri miyoyo ya ife tonse. Aka kadzakukhozetsani kuwona mmene. Baibulo lenilenilo limayankhira mafunso anu. Mboni za Yehova zidzakondwa kusonyeza, kwaulere, mmene makambitsirano oterowo angakhalire opindulitsa.

—AFALITSI

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena