Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • gh tsamba 3
  • Za M’katimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Za M’katimu
  • Mbiri Yabwino Yokusangalatsani
Mbiri Yabwino Yokusangalatsani
gh tsamba 3

Za M’katimu

TSAMBA MUTU

5 1 Kodi Mbiri Yabwino Ingapezeke Kuti Lero Lino?

10 2 Kupanga Bukhu la Mbiri Yabwino

19 3 Zimene Ziri m’Bukhu’lo

29 4 Chitsogozo Chopindulitsa ku Chimwemwe Cheni-cheni

39 5 M’mene Mbiri Yabwino Inasungidwira

48 6 Magwero a Mbiri Yabwino—“Mulungu”

58 7 Kulinganizira Anthu Malo Okhala Achimwemwe

66 8 Mlengi Aika Okhala pa “Chombo cha m’Mlengalenga Dziko Lapansi”

75 9 Uchimo Uchotsera Anthu Chimwemwe

85 10 Chimene Chimatichitikira Pamene Tifa

95 11 Mulungu Samazunza Miyoyo

106 12 Kodi N’chifukwa Ninji Mulungu Walola Kupanda Chimwemwe?

116 13 Chimasuko ku Imfa Kumka ku Moyo

124 14 Kulambira Mulungu Wamoyo

133 15 Kukhulupirira Malaulo Kungatsogolere ku Kupanda Chimwemwe

141 16 Kupanga Dziko Limodzi Pansi pa Ufumu wa Mulungu

151 17 Paradaiso wa Chisangalalo kaamba ka Anthu Onse

160 18 Mabanja Achimwemwe m’Chifuno cha Mulungu

166 19 Ana—“Cholandira cha kwa Yehova”

174 20 Njira ya Moyo Imene Imatsogolera ku Chimwemwe

183 21 Mulungu Apanga “Zinthu Zonse Kukhala Zatsopano”

TAMVERANI: Mau a Baibulo ogwidwa m’bukhu lino ngochokera mu Revised Untion Nyanja Version. Chizindikiro’cho NW chimasonyeza Baibulo lolembedwa’nso la 1971 la chinenero chamakono la New World Translation of the Holy Scriptures.

Ponena za madeti, chidule’cho B.C.E chimatanthauza “Nyengo Ino Isanakhale,” ndipo C.E chimatanthauza “A Nyengo Ino.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena