Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 158
  • Umodzi Wathu Wachikristu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Umodzi Wathu Wachikristu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Banja la Yehova Lili ndi Umodzi Wamtengo Wapatali
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Mgwirizano wa Akhristu Umalemekeza Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Sungani Umodzi m’Masiku Ano Otsiriza
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Umodzi Weniweni Wachikristu—Kodi Umatheka Motani?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 158

Nyimbo 158

Umodzi Wathu Wachikristu

(Aefeso 4:13)

1. Ndani ali ngati Yehova,

Magwerodi a umodzi!

Anatumizatu Mwana wake

Kudzatimasula ife.

Maziko a umodziwo

Anawaika mwa Kristu.

Kukhalatu monga banja limodzi

Ndi onse omvera Mawu.

2. Kodi ogwirizana n’Kristu

Tiri nalo thayo lanji?

Tikhale ndi khalidwe labwino,

Chifunocho chichitike.

Nkana tiri achisoni,

Mzimu umasangalatsa.

Muli chimwemwedi zedi m’kupatsa,

Potsanziratu Mulungu.

3. Wonani! teokrase Wake

E, atitchinjirizatu.

M’kulandira chowonadi chake,

Tidzakhala muumodzi.

M’lungu afunanji nafe?

Tisonye khalidwe lanji?

Kuchita chilungamo ndi chifundo,

Kuyenda modzichepetsa.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena