Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • la tsamba 2
  • Moyo Wokhutiritsa—Mmene Mungaupezere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Moyo Wokhutiritsa—Mmene Mungaupezere
  • Moyo Wokhutiritsa—Mmene Mungaupezere
Moyo Wokhutiritsa—Mmene Mungaupezere
la tsamba 2

Moyo Wokhutiritsa—Mmene Mungaupezere

Taganizirani zodabwitsa izi: M’dziko lina lotukuka, anthu oposa 90 peresenti amaona kuti ali ndi moyo wachimwemwe kwambiri kapena wachimwemwe chokwanira ndithu. Koma mitundu ya mankhwala itatu pa mitundu khumi yogwiritsidwa ntchito kwambiri m’dzikomo imaperekedwa kaamba ka vuto la kuvutika maganizo. M’dziko lokhalokhalo, 91 peresenti ya anthu amaona kuti moyo wa banja lawo uli wokhutiritsa. Chikhalirechobe, pafupifupi theka la maukwati kumeneko amatha!

Ndipo kufufuza anthu m’mayiko 18, okwana pafupifupi theka la chiŵerengero cha anthu onse padziko lapansi, kumaonetsa kuti “anthu ambiri padziko lapansi akuopa za m’tsogolo.” Choncho, n’chachidziŵikire kuti ambiri sali ndi moyo wokhutiritsa. Nanga inuyo bwanji? Kabukuka kalembedwa kuti kakuthandizeni kupanga moyo wanu kukhala wokhutiritsa kwenikweni.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena