Mutu wa Buku Lino/Tsamba la Ofalitsa
Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
Bukuli sitigulitsa. Timalipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo.
Ngati mukufuna kupereka pitani pawebusaiti yathu ya www.pr418.com/ny.
Malemba m’buku lino akuchokera m’Baibulo la Buku Lopatulika Ndilo Mau a Mulungu, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina. Komabe, Chichewacho tachilemba m’kalembedwe katsopano. Pamene tasonyeza NW, ndiye kuti lembalo lachokera m’Baibulo la New World Translation of the Holy Scriptures—With References
Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
Losindikizidwa mu October 2016
Learn From the Great Teacher
Chichewa (lr-CN)
© 2003
WATCH TOWER BIBLE AND TRACT SOCIETY OF PENNSYLVANIA