Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 4
  • Tipange Dzina Labwino kwa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tipange Dzina Labwino kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tipange Mbiri Yabwino kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kupanga Dzina Labwino ndi Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chifukwa Chake Tiyenera Kudziwa Dzina la Mulungu
    Dzina la Mulungu Limene Lidzakhala Kosatha
  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kugwiritsa Ntchito Dzina la Mulungu?
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 4

Nyimbo 4

Tipange Dzina Labwino kwa Mulungu

Losindikizidwa

(Mlaliki 7:1)

1. Pamoyo wathu, Tsiku lililonse

Tipange dzina Labwino kwa M’lungu.

Tikachita ntchito Zabwino kwa M’lungu,

Tisangalatsa Mtima wake.

2. Kufunitsitsa Kutchuka m’dzikoli,

Kufuna kuti Anthu atikonde

Kulibetu phindu Chifukwa Yehova

Sangatikonde Tikatero.

3. Tifuna M’lungu Atilembe dzina

Kuti tikhale, Mu buku la moyo.

Choncho tikhaletu Ndi dzina labwino

Kwa M’lungu wathu, Nthawi zonse.

(Onaninso Gen. 11:4; Miy. 22:1; Mal. 3:16; Chiv. 20:15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena