Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 11
  • Munachitira Ine Amene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Munachitira Ine Amene
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • “Munachitiranso Ine”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pemphero la Munthu Wovutika
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pemphero la Munthu Wovutika
    Imbirani Yehova
  • Ndithandizeni Ndikhale Wolimba Mtima
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 11

Nyimbo 146

Munachitira Ine Amene

(Mateyu 25:34-40)

  1. Nkhosa zina zomwe Yesu ali nazo,

    zimatumikira ndi odzozedwa.

    Zomwe nkhosa zina

    zingawachitire

    Yesu adzawabwezeratu zonse.

    (KOLASI)

    “Mwakuwatonthoza, mwanditonthoza.

    Zonse zimene munawachitira

    munachitiranso ine amene.

    Zonse zomwe munawachitira.

    munachitiranso ine amene.”

  2. “Pamene ndinali wanjala, waludzu,

    munandithandiza mwamsanga ndithu.”

    “Mbuye, tinachita

    liti zimenezi?”

    Ndiyeno Mfumu idzayankha kuti:

    (KOLASI)

    “Mwakuwatonthoza, mwanditonthoza.

    Zonse zimene munawachitira

    munachitiranso ine amene.

    Zonse zomwe munawachitira.

    munachitiranso ine amene.”

  3. “Zabwino mwachita mokhulupirika,

    polalikira ndi abale anga.”

    Choncho mfumuyo

    idzauza nkhosazo:

    “Landirani dziko, moyo wangwiro.”

    (KOLASI)

    “Mwakuwatonthoza, mwanditonthoza.

    Zonse zimene munawachitira

    munachitiranso ine amene.

    Zonse zomwe munawachitira.

    munachitiranso ine amene.”

(Onaninso Miy. 19:17; Mat. 10:40-42; 2 Tim. 1:16, 17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena