Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • lfb tsamba 4-5
  • Nkhani Zimene Zili M’bukuli

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’bukuli
  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
lfb tsamba 4-5

Zimene Zili M’bukuli

MUTU

Mawu Oyamba Gawo 1​—Ntchito Yolenga

1 Mulungu Analenga Kumwamba ndi Dziko Lapansi

2 Mulungu Analenga Mwamuna ndi Mkazi Oyamba

Mawu Oyamba Gawo 2​—Kuyambira Nthawi ya Adamu Mpaka Nthawi ya Chigumula

3 Adamu ndi Hava Sanamvere Mulungu

4 Kaini Anakwiya Mpaka Anapha M’bale Wake

5 Chingalawa cha Nowa

6 Anthu 8 Anapulumuka

Mawu Oyamba Gawo 3​—Kuyambira Nthawi ya Chigumula Mpaka Nthawi ya Yakobo

7 Nsanja ya ku Babele

8 Abulahamu ndi Sara Anamvera Mulungu

9 Anakhala ndi Mwana Atakalamba

10 Kumbukirani Mkazi wa Loti

11 Abulahamu Anasonyeza Kuti Anali Wokhulupirika

12 Yakobo Analandira Madalitso

13 Yakobo ndi Esau Anagwirizananso

Mawu Oyamba Gawo 4​—Kuyambira Nthawi ya Yosefe Mpaka pa Nyanja Yofiira

14 Kapolo Amene Ankamvera Mulungu

15 Yehova Sanaiwale Yosefe

16 Kodi Yobu Anali Ndani?

17 Mose Anasankha Kuti Azilambira Yehova

18 Anaona Chitsamba Chikuyaka

19 Miliri Itatu Yoyambirira

20 Miliri Inanso 6

21 Mliri wa 10

22 Zodabwitsa Zimene Zinachitika pa Nyanja Yofiira

Mawu Oyamba Gawo 5​—Aisiraeli Ali M’chipululu

23 Analonjeza Kuti Azimvera Yehova

24 Aisiraeli Sanachite Zimene Analonjeza

25 Chihema Cholambiriramo

26 Anthu 12 Anapita Kukafufuza Dziko la Kanani

27 Aisiraeli Ena Anaukira Yehova

28 Bulu wa Balamu Analankhula

Mawu Oyamba Gawo 6​—Oweruza

29 Yehova Anasankha Yoswa

30 Rahabi Anabisa Aisiraeli Okafufuza Dziko

31 Yoswa ndi Anthu a ku Gibiyoni

32 Mtsogoleri Watsopano Komanso Azimayi Awiri Olimba Mtima

33 Rute ndi Naomi

34 Gidiyoni Anagonjetsa Amidiyani

35 Hana Anapempha Mwana Wamwamuna

36 Zimene Yefita Analonjeza

37 Yehova Analankhula ndi Samueli

38 Yehova Anapatsa Mphamvu Samisoni

Mawu Oyamba Gawo 7​—Davide ndi Sauli

39 Mfumu Yoyamba ya Aisiraeli

40 Davide Anapha Goliyati

41 Davide ndi Sauli

42 Yonatani Anali Wolimba Mtima Komanso Wokhulupirika

43 Tchimo la Mfumu Davide

Mawu Oyamba Gawo 8​—Kuyambira Nthawi ya Solomo Mpaka Nthawi ya Eliya

44 Nyumba ya Yehova

45 Ufumu Unagawikana

46 Zimene Zinachitika Paphiri la Karimeli

47 Yehova Analimbikitsa Eliya

48 Mwana wa Mayi Wamasiye Anaukitsidwa

49 Mfumukazi Yoipa Inalangidwa

50 Yehova Anathandiza Mfumu Yehosafati

Mawu Oyamba Gawo 9​—Kuyambira Nthawi ya Elisa Mpaka Nthawi ya Yosiya

51 Kamtsikana Kanathandiza Mkulu wa Asilikali

52 Gulu Lamphamvu la Asilikali a Yehova

53 Yehoyada Anali Wolimba Mtima

54 Yehova Analezera Mtima Yona

55 Mngelo wa Yehova Anateteza Hezekiya

56 Yosiya Ankakonda Chilamulo cha Mulungu

Mawu Oyamba Gawo 10​—Kuyambira Nthawi ya Yeremiya Mpaka Nthawi ya Nehemiya

57 Yehova Anauza Yeremiya Kuti Azilalikira

58 Mzinda wa Yerusalemu Unawonongedwa

59 Anyamata 4 Amene Anamvera Yehova

60 Ufumu Umene Udzalamulire Mpaka Kalekale

61 Anakana Kulambira Fano

62 Ufumu Wofanana ndi Mtengo Waukulu

63 Dzanja Linalemba Pakhoma

64 Danieli Anaponyedwa M’dzenje la Mikango

65 Esitere Anapulumutsa Anthu a Mtundu Wake

66 Ezara Ankaphunzitsa Chilamulo cha Mulungu

67 Mpanda wa Yerusalemu Unamangidwanso

Mawu Oyamba Gawo 11​—Yohane M’batizi ndi Yesu

68 Elizabeti Anakhala ndi Mwana

69 Gabirieli Analankhula ndi Mariya

70 Angelo Analengeza za Kubadwa kwa Yesu

71 Yehova Anateteza Yesu

72 Zimene Yesu Anachita Ali Wamng’ono

73 Yohane Anakonza Njira

Mawu Oyamba Gawo 12​—Utumiki wa Yesu Padzikoli

74 Yesu Anakhala Mesiya

75 Mdyerekezi Anayesa Yesu

76 Yesu Anayeretsa Kachisi

77 Yesu Anakumana ndi Mayi Pachitsime

78 Yesu Ankalalikira Uthenga wa Ufumu

79 Yesu Anachita Zozizwitsa Zambiri

80 Yesu Anasankha Atumwi 12

81 Ulaliki wa Paphiri

82 Yesu Anaphunzitsa Otsatira Ake Kupemphera

83 Yesu Anadyetsa Anthu Ambiri

84 Yesu Anayenda Panyanja

85 Yesu Anachiritsa Munthu pa Tsiku la Sabata

86 Yesu Anaukitsa Lazaro

Mawu Oyamba Gawo 13​—Chakumapeto kwa Utumiki wa Yesu

87 Chakudya Chamadzulo Chomaliza

88 Yesu Anamangidwa

89 Petulo Anakana Yesu

90 Yesu Anaphedwa ku Gologota

91 Yesu Anaukitsidwa

92 Yesu Anakumana ndi Asodzi

93 Yesu Anabwerera Kumwamba

Mawu Oyamba Gawo 14​—Chikhristu Chinayamba Kufalikira

94 Ophunzira a Yesu Analandira Mzimu Woyera

95 Sanasiye Kulalikira

96 Yesu Anasankha Saulo

97 Koneliyo Analandira Mzimu Woyera

98 Anthu a Mitundu Ina Anamva Uthenga Wabwino

99 Woyang’anira Ndende Anaphunzira Mawu a Yehova

100 Paulo ndi Timoteyo

101 Paulo Anatumizidwa ku Roma

102 Zimene Yohane Anaona M’masomphenya

103 “Ufumu Wanu Ubwere”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena