Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 89
  • Mvera Kuti Udalitsidwe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mvera Kuti Udalitsidwe
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso
    Imbirani Yehova
  • Kodi Ndinu ‘Okonzeka Kumvera’?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Akamvera Adzapeza Moyo
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Akamvera Adzapeza Moyo
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 89

NYIMBO 89

Mvera Kuti Udalitsidwe

Losindikizidwa

(Luka 11:28)

  1. 1. Kodi timamveradi Yesu Khritsu

    Pa zonse zimene ananena?

    Zomwe anaphunzitsa ndi zabwino.

    Tikamumvera tidalitsidwa.

    (KOLASI)

    Mvera udalitsidwe

    Kuti usangalale.

    Zomwe Mulungu angakuuze,

    Mvera udalitsidwe.

  2. 2. Monga nyumba yomangidwa pathanthwe

    Osati yomangidwa pamchenga,

    Zochita zathu zingatiteteze

    Ngati timamvera Yesu Khristu.

    (KOLASI)

    Mvera udalitsidwe

    Kuti usangalale.

    Zomwe Mulungu angakuuze,

    Mvera udalitsidwe.

  3. 3. Monga mtengo wamumbali mwa madzi

    Umabereka mu nyengo yake,

    Tikamamvera tidzadalitsidwa.

    Tidzalandira moyo wosatha.

    (KOLASI)

    Mvera udalitsidwe

    Kuti usangalale.

    Zomwe Mulungu angakuuze,

    Mvera udalitsidwe.

(Onaninso Deut. 28:2; Sal. 1:3; Miy. 10:22; Mat. 7:​24-27; Luka 6:​47-​49.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena