Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm18 tsamba 2-3
  • Lachisanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lachisanu
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2018
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • MASANA
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2018
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2018
CO-pgm18 tsamba 2-3

Lachisanu

“Khala wolimba mtima kwambiri ndipo uchite zinthu mwamphamvu”​—YOSWA 1:7

M’MAWA

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 110 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YA TCHEYAMANI: Yehova Ndi Amene Amatithandiza Kuti Tikhale Olimba Mtima (Salimo 28:7; 31:24; 112:7, 8; 2 Timoteyo 1:7)

  • 10:10 NKHANI YOSIYIRANA: N’chifukwa Chiyani Akhristu Oona Amafunika Kulimba Mtima?

    • Kuti Azilalikira (Chivumbulutso 14:6)

    • Kuti Akhalebe Oyera (1 Akorinto 16:13, 14)

    • Kuti Asamalowerere Ndale (Chivumbulutso 13:16, 17)

  • 11:05 Nyimbo Na. 126 ndi Zilengezo

  • 11:15 KUWERENGA BAIBULO MWA SEWERO: “Limba Mtima, Ugwire Ntchitoyi Mwamphamvu”! (1 Mbiri 28:1-20; 1 Samueli 16:1-23; 17:1-51)

  • 11:45 “Chida Chilichonse Chimene Chidzapangidwe Kuti Chikuvulaze Sichidzapambana” (Yesaya 54:17; Salimo 118:5-7)

  • 12:15 Nyimbo Na. 61 ndi Kupuma

MASANA

  • 1:25 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:35 Nyimbo Na. 69

  • 1:40 NKHANI YOSIYIRANA: Zinthu Zolepheretsa Kukhala Wolimba Mtima Ndiponso Zinthu Zothandiza Kukhala Wolimba Mtima

    • Kutaya Mtima Ndiponso Chiyembekezo (Salimo 27:13, 14)

    • Mtima Wodandaula Ndiponso Mtima Woyamikira (Salimo 27:1-3)

    • Zosangalatsa Zosayenera Ndiponso Kulowa mu Utumiki (Salimo 27:4)

    • Kugwirizana Ndi Anthu Oipa Ndiponso Kugwirizana Ndi Anthu Abwino (Salimo 27:5; Miyambo 13:20)

    • Nzeru za Dziko Ndiponso Kuphunzira Patokha (Salimo 27:11)

    • Kukayikira Ndiponso Chikhulupiriro (Salimo 27:7-10)

  • 3:10 Nyimbo Na. 55 ndi Zilengezo

  • 3:20 NKHANI YOSIYIRANA: Anadalitsidwa Chifukwa Chokhala Okonzeka Kukumana Ndi Mavuto

    • Hananiya, Misayeli ndi Azariya (Danieli 1:11-13; 3:27-29)

    • Akula ndi Purisikila (Aroma 16:3 4)

    • Sitefano (Machitidwe 6:11, 12)

  • 3:55 “Limbani Mtima. Ine Ndaligonjetsa Dziko” (Yohane 16:33; 1 Petulo 2:21, 22)

  • 4:15 Asilikali Olimba Mtima a Khristu (2 Akorinto 10:4, 5; Aefeso 6:12-18; 2 Timoteyo 2:3, 4)

  • 4:50 Nyimbo Na. 22 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena