Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • scl tsamba 34-35
  • Kudziletsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kudziletsa
  • Malemba Othandiza pa Moyo wa Chikhristu
Malemba Othandiza pa Moyo wa Chikhristu
scl tsamba 34-35

Kudziletsa

Kodi Yehova amasonyeza bwanji kudziletsa?

Yer 18:7, 8; 2Pe 3:9

Kodi ndi mbali ziti pa moyo wathu zomwe timafunika kudziletsa?

Miy 16:32; 25:28; 1Ak 9:25, 27

Onaninso 2Ti 2:23-25; Tit 1:7, 8

  • Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:

    • 2Sa 16:5-14​—Mfumu Davide anadziletsa pamene Simeyi anamulankhula mawu onyoza komanso kumuchitira zinthu mopanda ulemu

    • 1Pe 2:21-23​—Mtumwi Petulo anafotokoza kuti Yesu anasonyeza kuleza mtima kwambiri pamene anthu ankamuchitira zachipongwe komanso kumuzunza

N’chiyani chingatithandize kuti tipitirize kudziletsa?

Lu 11:9-13; Aga 5:22, 23; Aef 4:23, 24; Akl 4:2

  • Nkhani za m’Baibulo zomwe zingakuthandizeni:

    • Lu 11:5-8​—Yesu anafotokoza kufunika kopitiriza kupempha kuti tithandizidwe

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena