Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w87 11/1 tsamba 32
  • Pangani Kuŵerenga Baibulo Kukhala kwa Tanthauzo Mokulira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pangani Kuŵerenga Baibulo Kukhala kwa Tanthauzo Mokulira
  • Nsanja ya Olonda—1987
Nsanja ya Olonda—1987
w87 11/1 tsamba 32

Pangani Kuŵerenga Baibulo Kukhala kwa Tanthauzo Mokulira

New World Translation of the Holy Scriptures​—With References m’chenicheni imapanga chimenechi.

Woŵerenga woyamikira posachedwapa analemba ponena za New World Translation Reference Bible: “Liri yankho ku mapemphero anga. Pamene ndipanga kuŵerenga kwanga kwa Baibulo, ndimafufuza zambiri za zilozerozo. Zimandithandiza ine kuwona maprinsipulo ena ofunika kwambiri amene ali ogwirizana ndi nkhaniyo. Icho mowonadi chimafutukula kumvetsetsa kwanga, ndipo ndingapange kugwiritsira ntchito kwaumwini kwabwinopo.”

Chofalitsidwa cha wophunzira chimenechi chiri chokutidwa ndi chikuto cholimba cha dark-maroon ndipo chiri ndi mawu a m’munsi oposa 11,000, indekisi yaikulu yosonyeza mawu enieni m’lembalo, ndi mapu. Kokha K72.00.

Chonde tumizani, mutalipiriratu positi, New World Translation of the Holy Scriptures​—With References. Ndatsekeramo K72.00. (Kunja kwa Zambia, lemberani nthambi ya Watch Tower ya kwanuko kaamba ka chidziŵitso.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena