Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w91 8/15 tsamba 32
  • M’mawa wa Bata

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • M’mawa wa Bata
  • Nsanja ya Olonda—1991
Nsanja ya Olonda—1991
w91 8/15 tsamba 32

M’mawa wa Bata

Zimenezo ndi zimene woŵerenga wa ku Illinois, U.S.A., ananena kuti magazini a Galamukani! amapereka. “Ndinadabwa mosangalatsidwa pambuyo poŵerenga kope la chofalitsidwa chanu cha Galamukani!” analemba motero munthuyo. “Mkazi wina ndiye anandipatsira magaziniyo m’mawa uno pa sitesheni ya sitima. Inandipangitsa kukhala wosanguluka ndi wamtendere, ndipo inali ndi chidziŵitso chothandiza. Chonde ndidziŵitseni mmene ndingamalandirire makope ameneŵa mokhazikika.

“Ndikuthokozaninso kaamba kondipatsa mmawa umodzi wa bata.”

Tikulingalira kuti nanunso mudzapindula ndi nkhani zosangalatsa za mu Galamukani! Ngati mungakonde kulandira magaziniŵa, tangodzazani ndi kutumiza kapepala kotsatiraka.

Ndingakonde kuti mudzinditumizira magazini a Galamukani! kunyumba kwanga. (Kunja kwa Zambia, lemberani ku nthambi ya Watch Tower yakumaloko kaamba ka chidziŵitso. Onani patsamba 2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena