Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w93 12/15 tsamba 31
  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1993

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1993
  • Nsanja ya Olonda—1993
  • Timitu
  • BAIBULO
  • LIPOTI LA OLENGEZA UFUMU
  • MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
  • MALO A KU DZIKO LOLONJEZEDWA
  • MBONI ZA YEHOVA
  • MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU
  • NKHANI ZA MOYO WA ANTHU
  • NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRIDWA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • YEHOVA
  • YESU KRISTU
Nsanja ya Olonda—1993
w93 12/15 tsamba 31

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1993

Zosonyezera deti la kope limene nkhaniyo ikupezeka

BAIBULO

Chitsogozo Chogwira Ntchito cha Munthu Wamakono, 5/1

Malo Otchulidwa m’Baibulo, 6/15

Maulosi a Baibulo, 5/15

Mbiri ya Baibulo, 6/1

Tifunikira Baibulo? 5/1

LIPOTI LA OLENGEZA UFUMU

2/1, 3/1, 5/1, 7/1, 8/1, 10/1, 11/1

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

Akristu ndi kuipitsidwa kwa malo, 1/1

Kodi Paulo akapereka moyo wake kaamba ka Ayuda? (Aroma 9:3), 9/15

Kuchita bizinesi ndi wosakhulupirira? 10/1

Kulephera kufika pa Chikumbutso, 2/1

Matikiti a mwaŵi, 6/15

Melikizedeke “wopanda maŵerengedwe a chibadwidwe chake,” (Aheb. 7:3), 11/15

Osakhulupirira amene afa chisautso chachikulu chisanayambe, 5/15

“Wopatsidwa mphatso ya mzimu” (1 Akor. 14:37), 10/15

Wosakhoza kupeza mnzake wamuukwati, 1/15

MALO A KU DZIKO LOLONJEZEDWA

Beeriseba, 7/1

Gerizimu, 1/1

Gilieadi, 9/1

Kondwerani! Nsupa Zisefukira Ndi Mafuta, 3/1

Nyanja ya Galileya, 11/1

Sinai​—Phiri la Mose ndi Chifundo, 5/1

MBONI ZA YEHOVA

Amishonale ku Micronesia, 3/1

Anamenyera Nkhondo Chikhulupiriro Chake (C. Bazán Listán), 6/15

Bwalo Lamilandu Lalikulu la Ulaya Lichilikiza Kuyenera kwa Kulalikira m’Greece, 9/1

Katundu Wachithandizo Asonyeza Chikondi Chachikristu (Russia, Ukraine), 2/1

Kulalikira Kumudzi ndi Mudzi ku Spain, 11/15

Kulalikira m’Dziko la Zinthu Zosiyanasiyana (Australia), 10/15

Kulalikira ndi Chipiriro m’Dziko la Madzi Oundana ndi la Moto (Iceland), 9/15

Kupeza Chuma Chenicheni mu Hong Kong, 5/15

Kutumba kwa Mtundu Wosiyana (Bahamas), 3/15

Limbikirani Muutumiki Waupainiya, 9/15

Maphunziro a Gileadi, 12/1

Misonkhano ya Chigawo ya “Chiphunzitso Chaumulungu,” 2/15

Misonkhano ya Chigawo ya “Onyamula Kuunika,” 1/15

Mulungu Samaiwala ‘Chikondi Chimene Munachiwonetsera’ (Eastern Europe), 1/1

“Olengeza Ufumu” Amaloŵa Pamadzi a Guyana, 4/1

Sukulu ya Gileadi​—Ya Zaka 50 Ndipo Ikupitabe Patsogolo! 6/1

Yehova Asanduliza Nthaŵi ndi Nyengo mu Romania, 6/15

Yehova Atetezera Anthu Ake mu Hungary, 7/15

MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU

Akristu Ayenera Kusunga Tsiku Lakupuma? 2/15

Amaŵeta Nkhosa Mwachifundo, 9/15

Chifukwa Chake Mufunikira Kufika Pamisonkhano Yachikristu? 8/15

Chikondi cha pa Mnansi, 9/15

Chiyembekezo​—Chinjirizo Lofunika, 4/15

“Funani Yehova, Ofatsa Inu Nonse,” 12/15

Khalani Achimwemwe ndi Adongosolo, 4/1

Kodi Mukuchita Zoposa? 4/15

Kodi Nkutumikiriranji Yehova? 5/15

Kodi Nkuvomereranji Cholakwa? 11/15

Kulankhulana​—Kuposa Kukambitsirana Chabe, 8/1

Kuphunzira Kuyembekezera, 10/15

Kusamalira Okalamba, 2/15

Kusunga Diso Lathu Lili “la Kumodzi” m’Ntchito Yaufumu, 12/15

Kuweta Nkhosa za Mtengo Wake za Yehova Mokoma Mtima, 7/15

Lamulo la Mkhalidwe Kapena Kutchuka? 10/1

Lingaliro Loyenera la Chifundo cha Mulungu, 10/1

Mfungulo ya Moyo Wabanja Wachipambano, 10/1

Mmene Akristu Angathandizire Okalamba, 8/15

Mmene Mungalimbitsire Zomangira Zaukwati, 8/15

Mpatsi wa “Mphatso Iliyonse Yabwino,” 12/1

Mulungu Amakulitsa​—Mumachita Mbali Yanu? 3/1

Mumalemekeza Malo Anu Olambirira? 6/15

Mumatsatira Yehova ndi Mtima Wonse? 5/15

Ulemerero wa Imvi, 3/15

Yehova Amakumbukira Odwala ndi Okalamba, 8/1

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

Choloŵa Chapadera Chachikristu (B. Brandt), 10/1

Kufupidwa ndi “Kolona wa Moyo” (F. Franz), 3/15

Kukula ndi Gulu la Yehova m’South Africa (F. Muller), 4/1

Kusindikiza Mabuku Ofotokoza Baibulo Mkati mwa Chiletso (M. Vale), 7/1

Kutumikira ndi Lingaliro la Kufulumira kwa Nthaŵi (H. van Vuure), 11/1

Kuyamikira Chichilikizo Chosalekeza cha Yehova (S. Gaskins), 6/1

Ndinapeza Chikhutiro Kutumikira Mulungu (J. Thongoana), 2/1

“Ndine Pano; Munditumize Ine” (W. John), 5/1

Yehova, Chidaliro Changa Kuyambira Paubwana Wanga (B. Tsatos), 8/1

Yehova Anandichirikiza m’Ndende ya m’Chipululu (I. Mnwe), 3/1

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRIDWA

Achichepere​—Kodi Mukulondola Chiyani? 4/15

Achimwemwe Ali Odzichepetsa, 12/1

Akristu ndi Chitaganya cha Anthu Lerolino, 7/1

Banja Lachikristu Limachitira Zinthu Pamodzi, 9/1

Banja Lachikristu Limaika Zinthu Zauzimu Poyamba, 9/1

Banja Lachikristu Limathandiza Okalamba, 9/1

Chenjerani ndi Nyimbo Zosayenera! 4/15

Chifundo cha Yehova Chimatipulumutsa Kukugwiritsidwa Mwala, 3/15

Chikondi (Agape)​—Zimene Sichili ndi Zimene Chili, 10/15

Chilakiko Chotsiriza cha Mikaeli, Kalonga Wamkulu, 11/1

Chilanditso pa Vumbulutso la Yesu Kristu, 5/1

Chilengedwe Chimati ‘Sangaŵiringule,’ 6/15

Chipiriro​—Nchofunika kwa Akristu, 9/15

Dalirani Yehova! 12/15

Dziŵani Yehova Kupyolera m’Mawu Ake, 6/15

‘Itanani Akulu,” 5/15

Khalani Olama m’Maganizo​—Mapeto Ayandikira, 6/1

Khalani Olimba Mtima! 11/15

Khalani Osandulika m’Maganizo ndi Ounikiridwa Mumtima, 3/1

Kodi Mulungu Amakudziŵanidi? 10/1

Kodi Ndani Amene Akutsatira Kuunika kwa Dziko? 4/1

Kodi Nkupeŵeranji Kulambira Mafano? 1/15

Kodi Tingawonjezere Motani Ukoma Pachikhulupiriro Chathu? 7/15

Kugonjera Kwaumulungu​—Chifukwa Ninji Ndipo ndi Yani? 2/1

Kukondwera mwa Mlengi Wathu Wamkulu, 1/1

Kukulitsa Mantha Aumulungu, 12/15

Kukulitsa Umunthu Watsopano mu Ukwati, 2/15

Kupeza Mfungulo ya Chikondi cha pa Abale, 10/15

Kutumikira Yehova ndi Mzimu Wodzimana, 6/1

Kuunikira Chidziŵitso pa Kukhalapo kwa Kristu, 5/1

Kuŵeta Limodzi ndi Mlengi Wathu Wamkulu, 1/1

Kuyenda Mwanzeru m’Dzikoli, 7/1

Labadirani Malonjezo a Mulungu mwa Kusonyeza Chikhulupiriro, 7/15

Lolani Kudziletsa Kwanu Kukhalepo Nikusefukire, 8/15

Masiku Aulosi a Danieli ndi Chikhulupiriro Chathu, 11/1

Mfumu Idetsa Malo Opatulika a Yehova, 11/1

“Mundisanthule, Mulungu”, 10/1

Musalole Aliyense Kukuipsirani Makhalidwe Anu Okoma, 8/1

Ntchito Zowonjezereka Mkati mwa Kukhalapo kwa Kristu, 5/1

Onyamula Kuunika​—Kaamba ka Chifuno Chotani? 1/15

Pambanani m’Kupeŵa Msampha wa Kusirira, 8/1

Peŵani Kulambira Mafano Kwamtundu Uliwonse, 1/15

Pitirizani Kukula m’Chidziŵitso, 8/15

“Pitirizanibe Kuyenda Monga Ana a Kuunika,” 3/1

Tsatirani Kuunika kwa Dziko, 4/1

“Ukwati Ukhaletu Wolemekezeka Pakati pa Onse,” 2/15

Ŵetani Gulu la Nkhosa la Mulungu Mofunitsitsa, 5/15

Wonjezerani Pachipiriro Chanu Kudzipereka Kwaumulungu, 9/15

Yehova Samapeputsa Mtima Wosweka, 3/15

Yendani Molimba Mtima m’Njira za Yehova, 11/15

Zimene Kugonjera Kwaumulungu Kumafuna kwa Ife, 2/1

Zitsanzo za Kudzichepetsa Zoyenera Kutsanziridwa, 12/1

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Akristu Oyambirira ndi Dziko, 7/1

Batizani! Batizani! Batizani!​—Koma Chifukwa Ninji? 4/1

Chikondi cha pa Ndalama, 2/15

Fodya ndi Atsogoleri Achipembedzo, 2/1

Helo, 4/15

Kodi Chabwino Chidzagonjetsadi Choipa? 2/1

Kodi Kuba Kudzatha Konse? 10/15

Kodi Kuthiridwa Mwazi Kumathokozedwa Mopambanitsa? 10/15

Kodi Mudzakwatulidwira Kumwamba? 1/15

Kodi Mumafunikiranji Kuti Mukhale Wachimwemwe? 6/1

Kodi Mungakhale ndi Moyo Kwautali Wotani? 11/15

Kodi Muyenera Kubatizidwa? 4/1

Kulemera Kungayese Chikhulupiriro Chanu, 7/15

Kuyeretsa Kwapadziko, 2/15

Kuzengereza Nkwakupha! 3/1

Masoka Achilengedwe, 12/1

“Mdani Wotsiriza” Adzagonjetsedwa! 11/15

Mgonero wa Ambuye, 3/15

Mkhalidwe Wamoyo wa Wodandaula Suli Wachimwemwe, 3/15

Mmene Dziko Lachikristu Linakhalira Mbali ya Dziko, 7/1

Ndodo Yachifumu ya Makangaza, 4/15

Papias Anaona Mawu a Ambuye Kukhala Amtengo Wapatali, 9/15

Peŵani Mzimu Wodzikweza! 5/15

Rahabi​—Anayesedwa Wolungama ndi Ntchito za Chikhulupiriro, 12/15

Sanaganize za Kulolera Molakwa! (Akristu Oyambirira), 11/15

Tchalitchi cha ku Latin America Chikuthedwa Nzeru, 6/15

Uchidakwa, 8/15

Utatu​—Kodi Umaphunzitsidwa m’Baibulo? 10/15

Zithumwa za Mwaŵi, 9/1

Zithunzithunzi Zachipembedzo, 4/15

Zolengedwa Zatsopano Zipangidwa! 1/1

YEHOVA

Akristu Oyambirira Anagwiritsira Ntchito Dzina la Mulungu? 11/1

Dzina la Mulungu, 12/1

Kodi Yehova Ndani? 7/15

Kuthetsa Chinsinsi cha Dzina Lalikulu Koposa, 11/1

Mlengi Wathu Wamkulu ndi Ntchito Zake, 1/1

Mpatsi wa “Mphatso Iliyonse Yabwino,” 12/1

Yehova​—Mulungu Wowona ndi Wamoyo, 7/15

Zochita za Yehova za Kupulumutsa Tsopano Lino, 12/1

YESU KRISTU

Kodi Anabadwa m’Nthaŵi ya Chipale? 12/15

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena