Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w96 12/15 tsamba 31
  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1996

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1996
  • Nsanja ya Olonda—1996
  • Timitu
  • BAIBULO
  • MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
  • MBONI ZA YEHOVA
  • MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU
  • NKHANI ZA MOYO WA ANTHU
  • NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA
  • YEHOVA
  • YESU KRISTU
Nsanja ya Olonda—1996
w96 12/15 tsamba 31

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1996

Zosonyeza deti la kope lopezekamo nkhaniyo

BAIBULO

Nkhondo Kaamba ka Baibulo la Chispanya, 6/1

Nthano ya Chigumula Imachirikiza Mbiri ya Baibulo, 9/15

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

Akristu amene ali ndi chiyembekezo cha padziko lapansi ali ndi mzimu wolingana ndi wa odzozedwa? 6/15

Atsopano akudzozedwa ndi mzimu woyera? 8/15

Chifukwa chake toʹte (pamenepo) amagwiritsiridwa ntchito kusonyeza choyambirira ndi chotsatira? 7/15

Dzina la banja lililonse (Aef 3:​14, 15), 1/15

Kodi Akristu angakhululukire machimo? 4/15

Kodi munthu akhoza kuiŵala chinthu modzifunira? (Afil 3:​13), 5/1

Kwanzeru kukaonana ndi sing’anga wa nthenda zamaganizo? 9/1

Ufumu wa Mulungu udze padziko lapansi? 6/1

Yesu akudziŵa deti la Armagedo? 8/1

MBONI ZA YEHOVA

Anachirikizidwa ndi Bwenzi Lawo Lalikulu Koposa (Czechoslovakia), 3/15

Chifutukuko ndi Dalitso la Yehova (kupatulira kumalikulu), 4/15

Kodi Ndinu Mpainiya Wolinganiza Zinthu? 5/15

Kufalitsa Choonadi cha Baibulo ku Portugal, 2/15

Kumaliza Maphunziro a Gileadi,6/1, 12/1

Kupuma Pantchito​—⁠Khomo Lotseguka la Ntchito Yateokrase? 7/15

Kuyenera kwa Chivomerezo Chodziŵa Kutsimikizidwanso, 11/15

Misonkhano Yachigawo ya “Atamandi Achimwemwe,” 1/15

Mkhalidwe Wochititsa Zinthu Kukula (Equatorial Guinea), 10/15

Mkupiti wa Umboni ku Greece, 4/15

Mtendere m’Dziko Lamavuto, 1/1

“Muzindikire Otere,” 6/15

“Ndiye Tchalitchi Chanu Chili Kuti?” (Mozambique), 12/15

Thangato Pakati pa Zowonongeka, 12/1

Ufulu wa Chipembedzo Uchirikizidwa ku Japan, 11/1

Umboni ku Cameroon, 8/15

Umboni ku Greenland, 6/15

Zoyenera za Wodwala Zilemekezedwa, 3/15

MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU

Chikristu Choyambirira ndi Boma, 5/1

Chitani Chikumbutso Moyenera, 4/1

Chitonthozo ndi Chilimbikitso​—⁠Ngale za Mbali Zambiri, 1/15

Gwiritsirani Ntchito Mwaŵi Wapadera Umenewu! 11/15

Kuchita Mogwirizana ndi Lumbiro Lanu la Ukwati! 3/1

Kukhala ndi Lingaliro Laumulungu pa Moŵa, 12/15

Kulunjika Nawo Bwino Mawu a Mulungu, 1/1

“Kumbukirani Masiku Apitawo”​—⁠Chifukwa Ninji? 12/1

Kupemphera Motani kwa Mulungu? 7/15

Kupeza Chimwemwe Popanga Ophunzira, 2/15

‘Kusamalira Nyumba ya Munthuwe’​—⁠m’Maiko Omatukuka, 10/1

Kutsanzira Mulungu Wathu Wopanda Tsankhu? 11/15

Kuuluka Pamwamba ndi Mapiko Monga Ziombankhanga, 6/15

Mmene Abusa Achikristu Amakutumikirirani, 3/15

Mphindi Yakutonthola ndi Mphindi Yakulankhula, 5/15

Mufunikiradi Kupepesa? 9/15

Mulungu, Boma, ndi Inuyo, 5/1

Yang’anani Kupyola pa Zinthu Zimene Mukuona! 2/15

Sungani Chidaliro Chili Cholimba Kufikira Mapeto, 5/1

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

Anatumikira Yehova Modzichepetsa (J. Booth), 6/15

Chiyembekezo cha Moyo Wanga Wonse​—⁠Kusafa Konse(H. Priest), 2/1

“Gwirirani Ntchito, Osati Chakudya Chimene Chimawonongeka” (D. Lunstrum), 4/1

Kutumikira Mulungu Wodalirika (K. Progakis), 9/1

Kutumikira Pansi pa Dzanja la Yehova Lachikondi (L. Zoumbos), 5/1

Kutumikira Yehova Monga Banja Logwirizana (A. Santoleri), 10/1

Kusumika Maso ndi Mtima pa Mphoto (E. Michael), 8/1

Mawu a Mulungu Amachita “Zozizwitsa” (T. Héon), 7/1

Ogwirizana mu Utumiki mu Nthaŵi Zabwino ndi Zoipa (M. and B. Muller), 3/1

Yehova Anakhala Nane (M. Henning), 6/1

Yehova Sanatisiye (N. Dori), 1/1

Yehova Wakhala Pobisalira Panga (P. Makris), 12/1

Zaka Zoposa 50 za ‘Kuwolokerako’’ (E. Paterakis), 11/1

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA

Achichepere Amene Amakumbukira Mlengi Wawo, 12/1

Achimwemwe Tsopano ndi Kosatha, 2/15

Anthu Afunikira Chidziŵitso Chonena za Mulungu, 1/15

Banja la Yehova Lili ndi Umodzi Wamtengo Wapatali, 7/15

‘Cherezani Alendo,’ 10/1

Chifukwa Chake Chipembedzo cha Dziko Chidzatha, 4/15

Chifukwa Chake Kulambira Koona Kumakhala ndi Dalitso la Mulungu, 4/15

Chilakiko cha Kulambira Koona Chayandikira, 7/1

Chilamulo cha Kristu, 9/1

Chilamulo Kristu Asanadze, 9/1

Dziperekeni pa Kuŵerenga, 5/15

Kachisi Wauzimu Wamkulu wa Yehova, 7/1

“Khalani Inunso Oyera Mtima m’Makhalidwe Anu Onse,” 8/1

Kodi Chachikulu Kopambana m’Moyo Wanu Nchiyani? 12/15

Kodi Mudzapulumuka Pamene Mulungu Achitapo Kanthu? 8/15

“Kondani Choonadi ndi Mtendere”! 1/1

Kuchereza Alendo Kwachikristu m’Dziko Logaŵanikana 10/1

Kudza kwa Yesu Kapena Kukhalapo kwa Yesu​—⁠Nchiti? 8/15

Kugaŵana Chitonthozo Chimene Yehova Amapereka, 11/1

Kukhala Mwamuna ndi Mkulu​—⁠Kulinganiza Mathayowo, 10/15

Kukhala Tate ndi Mkulu​—⁠Kukwaniritsa Mathayowo, 10/15

Khulupirirani Yehova ndi Mawu Ake, 2/1

Kupambana Chiyeso cha Kukhulupirika, 3/15

Kupereka Zake za Kaisara kwa Kaisara, 5/1

Kuphunzitsidwa Kuchita Chifuniro cha Yehova, 12/15

Kuthaŵira Kopulumukira “Chisautso Chachikulu” Chisanadze, 6/1

Kutsatira Chilamulo cha Kristu, 9/1

Madalitso Kapena Matemberero​—⁠Pali Chosankha! 6/15

Madalitso Kapena Matemberero​—⁠Zitsanzo kwa Ife Lerolino, 6/15

Makolo, Kondwerani mwa Ana Anu, 12/1

“Manja Anu Asakhale Olefuka” 3/1

Maphunziro​—⁠Agwiritsireni Ntchito Kutamanda Yehova, 2/1

Mbewu ya Njoka​—⁠Yavumbulidwa Motani? 6/1

Mmene Oyang’anira Oyendayenda Amatumikirira Monga Adindo Okhulupirika, 11/15

Mulungu ndi Kaisara, 5/1

“Mundilindire,” 3/1

‘Muyenera Kukhala Oyera Pakuti Ine Ndine Woyera,’ 8/1

Nkhosa za Yehova Zimafuna Kuzisamalira Mokoma Mtima, 1/15

‘Nyumba Yakupemphereramo Anthu a Mitundu Yonse,’ 7/1

Onse Ayenera Kudziŵerengera Mlandu kwa Mulungu, 9/15

Oyang’anira Oyendayenda​—⁠Mphatso mwa Amuna, 11/15

Pezani Chitonthozo kwa Yehova, 11/1

Sungani Umodzi m’Masiku Ano Otsiriza, 7/15

Tamandani Mfumu Yamuyaya! 4/1

“Tamandani Ya, Anthu Inu!” 4/1

Taonani Okhulupirika! 3/15

Tili ndi Chifukwa Chofuulira ndi Chimwemwe, 2/15

Ufumu wa Mulungu​—⁠Kodi Mukumvetsa Lingaliro Lake? 2/1

Umbeta​—⁠Khomo la Ntchito Yopanda Chocheukitsa, 10/15

Ŵerengani Mawu a Mulungu ndi Kumtumikira m’Choonadi, 5/15

Yehova Amapereka Mtendere ndi Choonadi Zochuluka, 1/1

Yehova Aŵerengeretu Bwino Mlandu Wanu, 9/15

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Achimwemwe m’Dziko Lopanda Chimwemwe 1/15

Akula ndi Priskila​—⁠Banja Lopereka Chitsanzo Chabwino, 12/15

Apolo​—Mlaliki wa Choonadi Chachikristu Wolankhula Mwanzeru, 10/1

Buthu Linalankhula Molimba Mtima, 5/15

Chisungiko Chenicheni​—⁠Chonulirapo Chovuta Kuchifikira, 5/15

Chisungiko Chenicheni​—⁠Tsopano ndi Kosatha, 5/15

Chitonthozo kwa Otsenderezedwa, 11/1

Chitonthozo Mkati mwa Zaka Zinayi za Nkhondo (Bosnia, Croatia), 11/1

Chiyembekezo Chabwino cha Sou, 8/1

Chiwawa Chili Ponseponse, 2/15

Chuma cha Solomo Nchokukumazidzwa? 10/15

Danieli Anatumikira Mulungu Mosalekeza, 11/15

Epafrodito​—⁠Nthumwi ya Afilipi, 8/15

Faraday​—⁠Wasayansi Ndiponso Mwamuna Wachikhulupiriro, 8/1

Filipo Abatiza Mdindo wa ku Aitiopiya, 7/15

Gamaliyeli​—⁠Anaphunzitsa Saulo wa ku Tariso, 7/15

Isitala Kapena Chikumbutso​—⁠Nchiti? 4/1

Kodi Baibulo Limaphunzitsa za Kukhulupirira Choikidwiratu? 9/1

Kodi Kuli Moyo Pambuyo pa Imfa? 10/15

Kodi Kusala Kudya Nkwachikhale? 11/15

Kodi Maloto Angalosere Mtsogolo? 10/1

Kodi Mtendere Ngwotheka? 1/1

Kodi Mulungu Amafuna Kusala Kudya? 11/15

Kodi Munapulumutsidwa? 2/1

Kodi Ndani Ayenera Kutchedwa Kuti Rabi? 7/1

‘Kodi Ndili Wofunika Pamaso pa Mulungu?’ 3/1

Kodi Sou Siimafa? 8/1

Kodi Tiyenera Kuchitanji Kuti Tipulumutsidwe? 2/1

Kubwerera Kufumbi​—⁠Motani? 9/15

Kukhala ndi Maubwenzi Okhalitsa, 3/15

Kutheratu kwa Chiwawa​—⁠Motani? 2/15

Kuunika Kuthetsa Nyengo ya Mdima, 1/15

Kuwonjezereka kwa Zochitika za Mbiri Yoipa, 4/15

Kuyendera Dziko Lolonjezedwa, 8/15

Lidiya​—⁠Wopembedza Mulungu Ndiponso Wochereza Alendo 9/15

Maphunziro Otengedwa ku Dziko Lolonjezedwa, 8/15

Mbiri Yabwino Mtsogolo! 4/15

Mmene Mulungu Amaonera Kulambira kwa Dziko Lachikristu, 7/1

Mose ndi Aroni​—⁠Alengezi Olimba Mtima, 1/15

Moyo Pambuyo pa Imfa​—⁠Motani, Kuti, Liti? 10/15

Moyo Wanu Umalamuliridwa ndi Choikidwiratu? 9/1

Ndi Wochitiridwa Tsankhu? 6/1

Nkumpatsiranji Yehova? 11/1

“Nyumba ya Davide”​—⁠Yeniyeni Kapena Yopeka? 10/15

Pamene Kugwa Masoka Achilengedwe, 12/1

Petro Alalikira pa Pentekoste, 9/15

Sikudzakhalanso Tsankhu! 6/1

Theophilus wa ku Antiokeya, 3/15

Tifunikira Mabwenzi Enieni, 3/15

“Tiphunzitseni Ife Kupemphera,” 7/15

Tiyenera Kulota, 10/1

Yona Aphunzira za Chifundo cha Yehova, 5/15

Zimene Zolengedwa “Zanzeru Mwachibadwa” Zimatiphunzitsa, 7/15

Zipembedzo Zonse Zimakondweretsa Mulungu? 9/15

OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA

1/1, 2/1, 3/1, 4/1, 5/1, 6/1, 8/1, 9/1, 10/1, 12/1

YEHOVA

Chifukwa Chake Iye Anagwiritsira Ntchito Dzina Lalikulululo, 4/15

Kodi Kukonda Mulungu Kumatanthauzanji? 6/15

Kodi Mungathe Kumkondadi Mulungu? 6/15

Mulungu Amasamala za Inu, 3/1

Mulungu Amavomereza Kulambira Kwamtundu Uliwonse? 7/1

Senzani Yehova Nkhaŵa Yanu Nthaŵi Zonse, 4/1

Yehova​—⁠Wokonda Chilungamo ndi Chiweruzo, 3/15

YESU KRISTU

Choonadi Ponena za Yesu, 12/15

Kodi Mukanamzindikira Mesiya? 11/15

Kulabadira Mawu a Yesu Otsazikira, 3/15

Uthenga Wabwino Malinga ndi Akatswiri, 12/15

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena