Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w08 4/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2008
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MLUNGU WA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO:
Nsanja ya Olonda—2008
w08 4/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 15, 2008

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MLUNGU WA:

May 26, 2008–June 1, 2008

Kanani Zinthu “Zopanda Pake”

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 48, 20

June 2-8, 2008

Mulungu Azikutsogolerani M’zinthu Zonse

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 131, 225

June 9-15, 2008

Achinyamata, Kumbukirani Mlengi Wanu Wamkulu

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 157, 183

June 16-22, 2008

Kukwatira Ndiponso Kukhala ndi Ana M’nthawi Yamapeto Ino

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 24, 164

June 23-29, 2008

Kodi Chofunika Ndi Chiyani Kuti Tikhale ndi Moyo Waphindu?

TSAMBA 21

NYIMBO ZOIMBA: 214, 67

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 3-11

Nkhani ziwirizi zikutithandiza kuzindikira “zinthu zopanda pake,” zinthu zomwe zingatilepheretse kutumikira Yehova. Zikufotokoza misampha imene ingathe kutikola mosavuta, ndipo zikupereka zifukwa zambiri zimene tiyenera kuyang’anira kwa Yehova kuti azititsogolera m’zinthu zonse.

Nkhani Zophunzira 3, 4 MASAMBA 12-20

Yoyamba ikuuza achinyamata kuti Baibulo lingawathandize kusankha zochita zimene zingasinthe moyo wawo. Yachiwiri ikuwapatsa malangizo abwino a m’Malemba a zimene ayenera kuganizira akafuna kukwatira kapena kukhala ndi ana.

Nkhani Zophunzira 5 MASAMBA 21-5

Nkhani yomalizayi ikufotokoza mfundo zochititsa chidwi za m’buku la Mlaliki. Ikutchula zinthu zofunikadi pamoyo, ndipo ikuzisiyanitsa ndi zinthu zimene dzikoli limalimbikitsa.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

Tisawaiwale Ngakhale Amakhala Kwaokha

TSAMBA 25

Kodi Mukukumbukira?

TSAMBA 29

Mawu a Yehova Ndi Amoyo Mfundo Zazikulu za M’buku la Yohane

TSAMBA 30

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena