Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w09 1/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2009
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO:
Nsanja ya Olonda—2009
w09 1/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 15, 2009

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

March 2-8, 2009

‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 200, 172

March 9-15, 2009

Sangalalani Ndi Ntchito Yopanga Ophunzira

TSAMBA  7

NYIMBO ZOIMBA: 130, 211

March 16-22, 2009

Kodi Ndinu ‘Mdindo wa Kukoma Mtima kwa m’Chisomo cha Mulungu’?

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 50, 58

March 23-29, 2009

Taonani Mtumiki Amene Yehova Amakondwera Naye

TSAMBA  21

NYIMBO ZOIMBA: 168, 4

March 30, 2009–April 5, 2009

Mtumiki wa Yehova “Analasidwa Chifukwa cha Zolakwa Zathu”

TSAMBA 25

NYIMBO ZOIMBA: 224, 214

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1-3 MASAMBA 3-16

Kodi kutsatira Khristu kumatanthauza chiyani? Kumatanthauza kutsanzira makhalidwe ake apadera monga nzeru ndi kudzichepetsa. Kumatanthauzanso kukhala achangu pantchito yopanga ophunzira. Ndiponso kumatanthauza kuwakonda zenizeni okhulupirira anzathu. Nkhani zimenezi zikufotokoza zimene tingachite potsanzira Khristu m’njira zitatu zimenezi.

Nkhani Zophunzira 4, 5 MASAMBA 21-29

Nkhani ziwiri zimenezi zikufotokoza maulosi angapo a m’buku la Yesaya amene anakwaniritsidwa pa Yesu Khristu. Kuphunzira maulosi amenewa kutithandiza kuyamikira kwambiri zimene Yehova ndi Yesu anatichitira mwa imfa ndi kuukitsidwa kwa Yesu. Choncho, nkhani zimenezi zitithandiza kuti tikonzekere m’maganizo ndi m’mitima yathu kuti tidzapezeke pamwambo wokumbukira imfa ya Yesu, umene udzachitike madzulo a pa April 9, 2009.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

“Njira Ndi Iyi, Yendani Inu Mmenemo”

TSAMBA 17

Mawu a Yehova Ndi Amoyo​—Mfundo Zazikulu za M’buku la Chivumbulutso​—Gawo 1

TSAMBA 30

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena