Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w09 4/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2009
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO:
Nsanja ya Olonda—2009
w09 4/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 15, 2009

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

June 1-7, 2009

Yobu Analemekeza Dzina la Yehova

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 197, 41

June 8-14, 2009

Umphumphu Wanu Umakondweretsa Mtima wa Yehova

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 160, 138

June 15-21, 2009

Chilengedwe Chimasonyeza Nzeru za Yehova

TSAMBA 15

NYIMBO ZOIMBA: 79, 84

June 22-28, 2009

Kuzindikira Mose Wamkulu

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 205, 150

June 29, 2009–July 5, 2009

Kuzindikira Yesu Monga Davide Wamkulu Ndiponso Solomo Wamkulu

TSAMBA 28

NYIMBO ZOIMBA: 168, 209

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

Nkhani Zophunzira 1, 2 MASAMBA 3-11

Nkhani zimenezi zikufotokoza chifukwa chake Yehova analola Satana kuti abweretsere Yobu mayesero osiyanasiyana. Zikufotokozanso chimene chinathandiza Yobu kusunga umphumphu wake. Komanso zikufotokoza zimene ifeyo tingachite kuti tikhalebe okhulupirika monga Yobu ndi kukondweretsa mtima wa Yehova.

Nkhani Yophunzira 3 MASAMBA 15-19

Zinthu zimene Yehova analenga zimasonyeza makhalidwe ake osiyanasiyana. Tingaphunzire zinthu zambiri ngati titamaganizira zimene iye analenga. M’nkhaniyi, tikambirana zinthu zinayi zimene Yehova analenga ndiponso zimene tingaphunzirepo.

Nkhani Zophunzira 4, 5 MASAMBA 24-32

Nkhani za m’Baibulo za anthu ena okhulupirika amene anakhalapo Yesu asanabadwe zimasonyeza kuti pali zinthu zina zofanana kwambiri pakati pa anthuwo ndi Yesu. M’nkhani ziwirizi, tikambirana za Mose, Davide ndi Solomo ndipo tiona mmene nkhani za moyo wawo zingatithandizire kuzindikira udindo wa Yesu pokwaniritsa cholinga cha Mulungu.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

Mafunso Ochokera kwa Owerenga​—Ngati mwana wabadwa wakufa, kodi pali chiyembekezo chakuti adzauka?

TSAMBA 12

Kodi Mukukumbukira?

TSAMBA 14

Kodi Mungakatumikire Kumene Kukufunika Ofalitsa Ufumu Ambiri?

TSAMBA 20

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena