Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 1/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 1/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

March 1-7, 2010

N’chifukwa Chiyani Muyenera Kudzipereka kwa Yehova?

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 7, 27

March 8-14, 2010

Ndife Anthu a Yehova Chifukwa cha Chisomo Chake

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 31, 16

March 15-21, 2010

Sonyezani Kuti Ndinu Wotsatira Weniweni wa Khristu

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 40, 25

March 22-28, 2010

Ulamuliro wa Satana Utha Posachedwa

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 46, 49

March 29, 2010–April 4, 2010

Yehova Ndiye Woyeneradi Kulamulira

TSAMBA 28

NYIMBO ZOIMBA: 30, 14

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 MASAMBA 3-11

Nkhani zimenezi zikufotokoza zimene kudzipereka kwa Yehova kumatanthauza ndiponso chifukwa chake tiyenera kudzipereka. Tikambirananso chifukwa chake sitiyenera kukayika kuti tingathe kuchita zimene Yehova amafuna. Komanso, tiona madalitso amene anthu onse a Yehova amapeza.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 MASAMBA 12-16

Nkhani imeneyi ikufotokoza mfundo zisanu zofunika kwambiri zimene tiyenera kuyesetsa kutsanzira Khristu. Tikamachita zimenezi, tidzasonyeza kuti ndife otsatira Khristu enieni, ndipo tidzatha kuthandiza anthu onga nkhosa kuzindikira mpingo woona wachikhristu.

NKHANI ZOPHUNZIRA 4, 5 MASAMBA 24-32

Nkhani yachinayi ikufotokoza chifukwa chake ulamuliro wa anthu wosadalira Mulungu walephera ndiponso mmene wasonyezera kuti ulamuliro wa Yehova ndi woyenera. Nkhani yachisanu ikufotokoza mmene tingasonyezere kuti tikuvomereza ulamuliro wa Yehova.

M’MAGAZINI INO MULINSO:

Thandizani Ana Anu Kulimbana ndi Mavuto Awo 16

Muzilemekeza Mulungu Tsiku ndi Tsiku 21

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena