Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 3/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 3/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

March 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

May 3-9, 2010

Kubatizidwa M’dzina la Atate, ndi la Mwana ndi la Mzimu Woyera

TSAMBA 10

NYIMBO ZOIMBA: 48, 7

May 10-16, 2010

Muziyenda mwa Mzimu Kuti Mukwaniritse Kudzipereka Kwanu

TSAMBA 14

NYIMBO ZOIMBA: 18, 51

May 17-23, 2010

“Olungama Adzawala Ngwee Ngati Dzuwa”

TSAMBA 19

NYIMBO ZOIMBA: 14, 30

May 24-30, 2010

Gulu Limodzi, Mbusa Mmodzi

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 30, 43

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 MASAMBA 10-18

Nkhani ziwirizi zitithandiza kumvetsa kufunika kwa kubatizidwa “m’dzina la Atate, ndi la Mwana ndi la mzimu woyera.” (Mat. 28:19) M’nkhanizi muli mfundo zimene zingakuthandizeni kukwaniritsa kudzipereka kwanu.

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 MASAMBA 19-28

M’fanizo lake la tirigu ndi namsongole, Yesu anafotokoza zimene zidzachitikire “ana a ufumu.” Kodi tirigu akuimira ndani, nanga namsongole akuimira ndani? Kodi fanizo limeneli likukwaniritsidwa bwanji masiku ano? Kodi limangonena za odzozedwa okha?

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

Khalanibe Paubwenzi ndi Mulungu Ngakhale Zinthu Zitasintha 3

Maliko ‘Anali Wofunika Potumikira’ 6

Mafunso Ochokera kwa Owerenga 28

Khalanibe ‘Oyera Mtima’ Masiku Ovuta Ano 30

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

By permission of the Israel Museum, Jerusalem

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena