Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 4/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 4/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

May 31, 2010–June 6, 2010

Achinyamata, Khalani ndi Mtima Wokonda Kwambiri Kutumikira Yehova

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 11, 41

June 7-13, 2010

Ntchito ya Mzimu Woyera Pokwaniritsa Cholinga cha Yehova

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 43, 19

June 14-20, 2010

Musamaone Zinthu Zachabe

TSAMBA 20

NYIMBO ZOIMBA: 29, 52

June 21-27, 2010

Kodi Mukutsatira Khristu ndi Mtima Wonse?

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 54, 17

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI YOPHUNZIRA 1 MASAMBA 3-7

Yehova akuuza achinyamata kuti azimvera, kuphunzira ndi kutsatira malangizo ake. Nkhaniyi ikufotokoza mmene kuwerenga Baibulo, kupemphera ndiponso khalidwe labwino zingathandizire achinyamata kulambira Yehova ndi mtima wonse.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 MASAMBA 7-11

Tikudziwa kuti cholinga cha Yehova chidzakwaniritsidwa ndipo palibe chimene chingalepheretse. Nkhaniyi ikufotokoza ntchito ya mzimu woyera pokwaniritsa cholinga cha Yehova m’nthawi yakale, masiku ano komanso m’tsogolo.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 MASAMBA 20-24

Pamene dziko la Satanali likuyandikira mapeto ake, timaona ndiponso kumva zinthu zimene zingasokoneze ubwenzi wathu ndi Mulungu. M’nkhani ino tikambirana zina mwa zinthu zimenezi, chifukwa chake Satana amazigwiritsa ntchito komanso zimene tingachite kuti tidziteteze.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 MASAMBA 24-28

Kodi n’chiyani chingatithandize kukhalabe achangu potumikira Mulungu? Ngati tikufuna kupitirizabe kutsatira Khristu, kodi tiyenera kupewa chizolowezi chiti? Nkhaniyi ikufotokoza mayankho a mafunso ofunika amenewa.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

Kodi Mukukumbukira? 12

Kodi Mumalola Yehova Kukufunsani Mafunso? 13

Mavuto Amene Takumana Nawo Atithandiza Kudalira Yehova 16

Yehova Amafuna Kuti Mukhale Otetezeka 29

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena