Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 6/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 6/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

June 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

July 26, 2010–August 1, 2010

Khalani Otetezeka M’gulu la Anthu a Mulungu

TSAMBA 6

NYIMBO ZOIMBA: 16, 31

August 2-8, 2010

Muzilimbikitsana Mumpingo

TSAMBA 10

NYIMBO ZOIMBA: 50, 53

August 9-15, 2010

“Pitirizani Kugonjetsa Choipa” mwa Kupewa Kupsa Mtima

TSAMBA 15

NYIMBO ZOIMBA: 52, 39

August 16-22, 2010

Kulankhula Mwaulemu Kumathandiza Kuti Tizikhala Bwino ndi Ena

TSAMBA 20

NYIMBO ZOIMBA: 19, 35

August 23-29, 2010

Kuchita Zinthu Zauzimu Kumatsitsimula

TSAMBA 25

NYIMBO ZOIMBA: 22, 48

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 MASAMBA 6-14

Nkhani zimenezi zitithandiza kuti tiziyamikira kwambiri madalitso amene timapeza chifukwa chokhala mumpingo wachikhristu. Mulinso mfundo zimene zingatithandize ifeyo patokha kuona mmene tingathandizire abale ndi alongo anthu mumpingo.

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 MASAMBA 15-24

Nkhani ziwiri zimenezi zikufotokoza mmene kutsatira mfundo za m’Baibulo kungatithandizire kukhala mwamtendere ndi anthu ena ngakhale kuti tonse ndife opanda ungwiro. Zikufotokozanso kuti kulankhulana mwaulemu kungathandize kwambiri kuti tizikhala bwino ndi anthu.

NKHANI YOPHUNZIRA 5 MASAMBA 25-29

Nkhani imeneyi itithandiza kudziwa mmene tingapezere chimwemwe chosatha ndiponso chokhalitsa. Anthu m’dzikoli ali ndi maganizo olakwika pa zinthu zimene zimatsitsimula ndipo amakonda kwambiri zofuna za mtima wawo. Koma anthu a Mulungu amatsitsimulidwa akamachita zinthu zauzimu.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

Ogwirizana Chifukwa cha Chikondi Lipoti la Msonkhano Wapachaka 3

Zimene Mungachite Ngati Mwamuna Kapena Mkazi Wanu Ali Wosakhulupirika 29

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena